Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Mafumu Ati Adzigwira Ntchito Limodzi ndi Boma

$
0
0

Mfumu yayikulu Mbenje ya m’boma la Nsanje yalangiza mafumu m’dziko muno kuti adzigwira ntchito limodzi ndi boma lomwe likulamula ndi cholinga chofuna kulimbikitsa ntchito za chitukuko m’dziko lino.

Mfumuyi imalankhula izi pa mwambo wokweza Nyakwawa Kadamila kukhala a Group Village Headman ya mdela lake. Iwo ati mafumu akuyenera kumadzipeleka pa ntchito zotumikira boma lomwe likulamula pofuna kupititsa patsogolo ntchito yotukula dziko lino. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>