Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Atsogoleri a mdziko la Nigeria Ateteze Maufulu a Anthu

$
0
0

Ma episkopi a mpingo wa katolika m’dziko la Nigeria apempha atsogoleri a dzikolo kuti ayesetse kuteteza ufulu wa anthu m’dzikomo.

Malingana ndi malipoti a Catholic News Agencyma episkopiwa alankhula izi atachita zokambilana masiwa apitawa.

Iwo ati dzikolo likukumana ndi mavuto osiyanasiyana monga a umphawi ndi za mtopola zomwe gulu la zauchifwamba la Boko Haramu ndi magulu ena a zauchifwamba akulimbikitsa m’dzikomo.

Iwo alangiza mzika za dzikolo kuti zikhale zogwirizana pofuna kuthana ndi mavutowa.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>