Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Mphunzitsi Amangidwa Kamba Kogwilirira Mwana wa Sukulu

Apolisi m’boma la Ntchisi amanga mphunzitsi wa pa sukulu ina ya pulayimale kamba kogwirira ophunzira wina pa sukulupo wa zaka 16 zakubadwa. Mneneri wa apolisi m’bomalo Sergent  Gladson M’bumpha...

View Article


Dayosizi Ya Mangochi Ilimbikitsa Ana Kupewa Malungo

Dayosizi ya mpingo wa katolika ya Mangochi kudzera mu nthambi yoona za umoyo ya Catholic Health Commission mu dayosiziyo yati ipitiriza kuphunzitsa ana njira zimene angapewere matenda a malungo. Vicar...

View Article


Apempha Amayi Azitanganidwa Kukweza Dziko, Miyoyo Yawo

Amayi ochokera m’mipingo yosiyanasiyana m’dziko muno awapempha kuti azikonda kutanganidwa ndi zinthu zomwe zingathandize pa chitukuko cha miyoyo yawo ndi dziko lino. Mayi Trizer Masauli omwe...

View Article

Amayi a Katolika Awapempha Azamitse Moyo wa Mapemphero

Amayi a chikatolika mu arkidayosizi ya Blantyre awapempha kuti azamitse moyo wawo wa mapemphero ngati njira imodzi yosinkhasinkha moyenera masautso a ambuye yesu khristu. Mlembi wa za utumiki mu...

View Article

Ma Episkopi Mdziko la South Africa Adzudzula Ziwawa Mdzikolo

Maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la South Africa adzudzula  mchitidwe wa ziwawa omwe ukuchitika mdzikolo potsatira chisankho cha makhansala chomwe chikuyembekezeka kuchitika mwezi wa mawa. Malinga...

View Article


Atsogoleri a mdziko la Nigeria Ateteze Maufulu a Anthu

Ma episkopi a mpingo wa katolika m’dziko la Nigeria apempha atsogoleri a dzikolo kuti ayesetse kuteteza ufulu wa anthu m’dzikomo. Malingana ndi malipoti a Catholic News Agencyma episkopiwa alankhula...

View Article

Papa Akumana ndi Pulezidenti wa Dziko la Lebanon

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco ati anachita zokambirana ndi mtsogoleri wa dziko la Lebanon Michel Aoun yemwe anakayendera likulu la mpingo wakatolikali. Malinga ndi...

View Article

Anthu Asamalire Chilengedwe Pofuna Kupewa Njala

Anthu mdziko muno ati akuyenera kutenga mbali yaikulu yoteteza chilengedwe pofuna kupewa vuto la kusowa kwa chakudya lomwe padakali pano lakhudza kwambiri dziko la Malawi. Vicar General wa dayosizi ya...

View Article


Woyimira Anthu pa Milandu Wapezeka Atafa Mdziko la Kenya

Loya wina yemwe amayimilira  munthu wina pamlandu woti apolisi m`dziko la Kenyaakumachitira nkhanza  anthu m`dzikolo wapezeka  atafa munzinda wa Nairobi m`dzikolo. Loyayu, Willie Kimani wa zaka 32,...

View Article


Ma Episkopi Mdziko la South Africa Adzudzula Ziwawa Mdzikolo

Maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la South Africa adzudzula  mchitidwe wa ziwawa omwe ukuchitika mdzikolo potsatira chisankho cha makhansala chomwe chikuyembekezeka kuchitika mwezi wa mawa. Malinga...

View Article

Chitukuko Chingapite Patsogolo Ngati Adindo ndi Mzika Akulumikizana

Kulumikizana pa nkhani za chitukuko cha m’madera pakati pa adindo komanso mzika ati ndi njira yokhayo yomwe ingapititse patsogolo chitukuko cha dziko lino. Wachiwiri kwa mfumu ya mzinda wa Blantyre, a...

View Article

President wa Dziko la Phillipines Wakana Maukwati a Amuna, Akazi Okhaokha

Mtsogoleri wa dziko la Phillipines Rodrigo Duterte wakanitsitsa kuvomeleza maukwati a amuna kapena akazi okhaokha. Malipoti a wailesi ya BBC mtsogoleriyu wakanitsitsa kuti sangavomereze mchitidwewu...

View Article

Papa Apempha Ansembe Ayike Patsogolo Sakramenti la Kulapa

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisko wapempha ansembe kuti ayike sakramenti la kulapa patsogolo kuti alimbikitse umoyo wa uzimu mma parishi mwawo. Papa Francisko amalankhula...

View Article


Ambuye Msusa Apempha Amayi Azipereke Potukula Uzimu

Arkiepiskopi wa arkidayosizi ya mpingo wa katolika ya Blantyre Ambuye  Thomas Luke Msusa walimbikitsa amayi mu arkidayisizi-yi kuti azipeleke potukula uzimu pakati pa anthu. Ambuye Msusa apeleka...

View Article

Maepiskopi Mdziko la USA ati Miyoyo ya Anthu Osauka ili pa Chiopsezo

Maepiskopi a mpingo wa katolika mdziko la United States of America ati miyoyo ya anthu ovutika mdzikolo ili pa chiopsezo potsatira ndondomeko yatsopano ya zaumoyo yomwe yakhazikitsidwa mdzikolo....

View Article


Papa Wapepesa Anthu Amene Akhuzidwa Ndi Chiwembu Mdziko la Bangladesh

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko wapereka uthenga wa chipepeso kwa anthu omwe akhudzidwa ndi chiwembu chomwe chaphetsa anthu makumi awiri mu mzinda wa Dhaka mdziko la...

View Article

Mutharika Wati Atukula Mzinda wa Zomba

President wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati boma lake likhazikitsa zitukuko zosiyanasiyana mu mzinda wa Zomba ndi cholinga choti mzindawu udzifanafana ndi mizinda ina ya mdziko...

View Article


Apempha Wailesi Zifalitse Nthenga Wothetsa Kufala Kwa Kolera

Nyumba zowulutsa mawu za m’madera a kumidzi (Community Radio) azipempha kuti zizipereke pa ntchito yofalitsa mauthenga a njira zopewera matenda a kolera omwe amafala kwambiri mu nyengo ya mvula....

View Article

Kaliati Apempha Mabanja Athandize Radio Maria Malawi

Nduna ya zophunzitsa anthu mai Patricia Kaliati wapepha mabanja kuti athandizire Radio Maria Malawi kufalitsa nthenga wa chipulumutso mu njira zosiyanasiyana. Mai Kaliati amalankhula izi ku parish ya...

View Article

Dayosizi ya Mangochi Ikufuna Akhristu Apindule ndi Nyumba Zake Zowulutsira Mawu

Dayosizi ya mpingo wa katolika ya Mangochi yati ikufuna igwiritse bwino ntchito nyumba zowulutsira mawu zomwe ili nazo pofalitsa nthenga wa Mulungu. Episkopi wa dayosiziyi Ambuye Montfort Stima ndi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>