Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Alimbikitsa Akhristu Kukhala Ozidalira

$
0
0

Episikopi  wa Mpingo wakatolika mu Dayosizi ya Zomba Olemekezeka Ambuye George Desmond Tambala wapempha Akhristu aku Tchalitchi cha Matawale chomwenso ati posachedwapa akufuna kuchikhadzikitsa kukhala  Parish mu Dayosizi-yi kuti akhale odzidalira.

Ambuye Tambala anena idzi Lamulungu lapitali pambuyo pa mwambo wa nsembe ya Ukaristia pomwe  anapita kukayendera akhristu a tcharichiri. Ambuye Tambala athokozanso akhristu a ku Matawale chifukwa chomanga nyumba  yamakono komanso yaikulu yopemphereramo. Iwo ati izi zawapatsa chilimbikitso kuti  mtsogolomu akhala akukhadzikitsa tchalichiri kukhala parish  ndipo ati udzakhala mpingo odzidalira pawokha pazachuma. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>