Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Mphunzitsi Azipha Pozimangilira M’boma la Dedza

$
0
0

Bambo wina wa zaka 47zakubadwawadzipha podzimangilira m’boma la Dedza.

Malingana ndi ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Edward Kabango, bambo-yu ndi Ives Kumankhamba ndipo anali mphunzitsi pa sukulu ya pulayimale ya Buam’bomalo.

Malemuyi akuti wadzipha mkazi wake anali kumudzi komwe amakazonda odwala. Padakalipano  gwero la imfa ya mkulu-yi silikudziwika.

Malemu Ivesi Kumankhamba amachokera m’mudzi mwa Fosa kwa mfumu yaikulu Kachere m’boma lomwelo la Dedza.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>