Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Dziko la Iraq Lakhazikitsa Komiti Yodzetsa Chitetezo

$
0
0

Nduna yayikulu ya dziko la Iraq yakhazikitsa komiti yomwe izigwira ntchito yoteteza akhristu komanso madera ena omwe amayang’aniridwa ndi boma m’dzikolo.

Ndunayi    yakhazikitsa komitiyi potsatira  pempho la mtsogoleri wa maepiskopi mdzikolo Patriarch Louis Raphael Sako yemwe wapempha boma kuti liteteze akhristuwa omwe akukumana ndi nkhanza zosiyanasiyana kuchokera ku magulu a ziwembu.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>