Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ntchito Zoweruza Milandu Ziyamba Kuyenda Mwachangu

Ntchito zoweruza milandu mmabwalo osiyanasiyana mdziko muno ati ziyamba kuyenda mwachungu potsatira kusintha kwa zipangizo  zogwilira ntchitoyi zomwe mabwalo aakulu alandira mdziko muno. Mmodzi mwa...

View Article


Papa Francisco Apepesa Mabanja omwe Ataya Abale Mdziko la China

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco wapereka uthenga opepesa ku mabanja omwe ataya abale awo pangozi yomwe yachitika mdziko la China makina a fakitore ina ataphulika mchigawo...

View Article


Kadinala Njue Wapempha Anthu a Mdziko la Kenya kuti Akhale a Makhalidwe Abwino

Kadinala John Njue wa m’dziko la Kenya wapempha m’zika za dziko la kwawo  zomwe zikukhala m’dziko la America kuti zisamatengere  makhalidwe oyipa omwe mzika zina zimachita m’dzikomo.   Kadinala Njue...

View Article

Mayi wa Zaka 50 Wadzipha

Mayi wina wa zaka 50 m’boma la Ntchisiwadzipha podzimangilira ku mtengo kamba koti anapezeka ndi matenda a khansa.   Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergent Gladson M’bumpha watsimikiza za...

View Article

Pulezidenti Kiir Asayinira Pangano la Mgwirizano

Mtsogoleri wadziko la South Sudan A Salva Kiir wati asayinira mgwirizano odzetsa mtendere pakati pa iye ndi magulu owukira boma mdzikolo. Pulezidenti Kiir lolemba analonjeza kuti asainira panganoli...

View Article


Bungwe la MEC Lichititsa Chisankho Chapadera

Bungwe loyendetsa zisankho mdziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lachiwiri lichititsa chisankho chapadera cha makhansala mmadera asanu  momwe mulibe makhansala pazifukwa zosiyanasiyana...

View Article

Apolisi m’boma la Dowa Agwira Mzika za Mdziko la Ethiopia

Apolisi m’boma la Dowa amanga mzika zisanu ndi zinayi za mdziko la Ethiopia zomwe zalowa mdziko muno popanda zitupa zoyenera.   Apolisi m’bomalo agwira anthuwa usiku wa lamulungu lapitali atawapeza...

View Article

Zigawenga Zisanu za Boko Haram Zaphedwa

Anthu asanu a mgulu la zigawenga za Boko Haram aphedwa ndi asilikali a boma mdziko la Nigeria.   Asilikaliwo apha zigawengazo zitachitira chiwembu mdipiti wa galimoto za asilikali zomwe zimaperekeza...

View Article


Dziko la France Lipereka Ulemu kwa Omwe Ateteza Sitima ku Zauchifwamba

Dziko la France lolemba lapereka ulemu wapadera kwa mzika zitatu za mdziko la America ndi ina yaku Britain chifukwa cholepheretsa munthu wina wamgulu la zaufwamba yemwe amafuna kupha anthu mu sitima...

View Article


Boma Likhazikitsa Malo a Achinyamata Ophunziliramo Ntchito ZamanjaBoma...

Mlangizi wa pulezidenti pankhani za mabungwe a Mavuto Bamusi atsimikizira mabungwe omwe siaboma m’boma la Zomba kuti boma likhazikitsa malo oti achinyamata aziphunziliramo ntchito za manja m’boma...

View Article

Bungwe la UN Lawopseza Dziko la South Sudan

Bungwe la United Nations (UN) lawopseza kuti lichitapo kanthu ngati mtsogoleri wa dziko  la South Sudan a Salva Kiir  sasayina pangano la mtendere ndi magulu omwe akuwukira dzikolo. Pa msonkhano wa...

View Article

Dziko la USA Lachenjeza Dziko la South Sudan kuti Lisaphwanye Pangano

Dziko la United States lachenjeza  atsogoleri  a dziko la South Sudan kuti asaphwanye pangano lomwe asayinira lomwe cholinga chake ndi kuthetsa nkhondo ya pachiweniweni yomwe yakhala ikuchitika...

View Article

Dziko la Iraq Lakhazikitsa Komiti Yodzetsa Chitetezo

Nduna yayikulu ya dziko la Iraq yakhazikitsa komiti yomwe izigwira ntchito yoteteza akhristu komanso madera ena omwe amayang’aniridwa ndi boma m’dzikolo. Ndunayi    yakhazikitsa komitiyi potsatira...

View Article


Maepiskopi Mdziko la France Adzudzula Anthu omwe Atentha Mzikiti Mdzikolo

Bungwe la maepiskopi mdziko la France ladzudzula anthu ena omwe atentha mzikiti mtauni ina kum’mwera chakumvuma mdzikolo masiku apitawa. Muuthenga omwe bungweli latulutsa maepiskopiwo ati zomwe achita...

View Article

Anthu Oposera 100 Afa mu Nyanja ya Mediterranean

Anthu oposera 100 akuwaganizira kuti afa mdziko la Libya mabwato awiri omwe anakwera  atamila munyanja ya Mediterranean pomwe amapita mmayiko aku ulaya. Malinga ndi akuluakulu a boma mdziko la Libya...

View Article


Bungwe la Eye of the Child ndi Lokhudzidwa ndi Imfa ya Mwana wa Zaka Zisanu

Bungwe la Eye of the Child lati ndi lokhudzidwa kwambiri ndi imfa ya mwana wazaka zisanu yemwe waphedwa masiku apitawa mumzinda wa Lilongwe pofuna kugwiritsa ntchito ziwalo zake ngati zizimba...

View Article

Dziko la Egypt Lidzudzula Kazembe wa M’dziko la Britain

Dziko la Egypt linayitanitsa kazembe wa dziko la Britain mdzikolo John Casson, chifukwa chodzudzula bwalo la milandu mdzikolo lomwe lalamula atolankhani atatu a wailesi ya kanema ya Al-Jazeera kuti...

View Article


Asilikali a Dziko la South Sudan Aphwanya Pangano

Asilikali owukira boma mdziko la South Sudan adzudzula asilikali a boma mdzikolo chifukwa chophwanya pangano la mtendere lomwe atsogoleri ambali ziwirizi asayinira masiku apitawa asilikaliwo...

View Article

Anthu Awiri Afa ndipo Ena 9 Avulala pa Ngozi ya Galimoto M’boma la Zomba

Anthu awiri afa ndipo ena asanu ndi anayi avulala minibus yomwe anakwera itagubuduzika  dalaivala wake atalephera kuwongolera m’boma la Zomba.   Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali a Patricio Supriano...

View Article

Anthu Khumi Afa ndi Moto Mdziko la France

Anthu khumi afa ndi ena anayi avulala kodetsa nkhawa ndi moto omwe unabuka mwadzidzi mu nyumba ina mu mzinda wa  Paris mdziko la France. Malinga ndi malipoti a wayilesi ya BBC chomwe chinayambitsa...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>