M’tsogoleri wa dziko la America a Barack Obama wati dziko la America liyesetsa pothana ndi magulu a zigawenga omwe akulimbikitsa ziwembu m’mayiko osiyanasiyana.
Iye walakhula izi pokhudzidwa ndi imfa ya anthu khumi ndi anayi omwe aphedwa pa chiwembu chomwe magulu ena a zauchifwamba achititira anthu okhala ku San Bernardino m’dzikomo.
Iye wati zomwe zachitikazi ndi zokhudza kwambiri choncho mkofunika kuti dziko lake litengepo mbali pa ntchito zowonetsetsa , kuti anthu a m’dzikomo akukhala mwa bata ndi mtendere.
Magulu a zigawenga omwe padakali pano ndi amene akusowetsa mtendere m’mayiko osiyanasiyana ndi monga la Islamic State IS lomwe linakachitanso chiwembu ndi kupha anthu oposera zana limodzi mdziko la France la Boko Haram m’dziko la Nigeria ndinso la Al Shabaab m’dziko Somalia.
M’tsogoleri wa dziko la America a Barack Obama wati dziko la America liyesetsa pothana ndi magulu a zigawenga omwe akulimbikitsa ziwembu m’mayiko osiyanasiyana.
Iye walakhula izi pokhudzidwa ndi imfa ya anthu khumi ndi anayi omwe aphedwa pa chiwembu chomwe magulu ena a zauchifwamba achititira anthu okhala ku San Bernardino m’dzikomo.
Iye wati zomwe zachitikazi ndi zokhudza kwambiri choncho mkofunika kuti dziko lake litengepo mbali pa ntchito zowonetsetsa , kuti anthu a m’dzikomo akukhala mwa bata ndi mtendere.
Magulu a zigawenga omwe padakali pano ndi amene akusowetsa mtendere m’mayiko osiyanasiyana ndi monga la Islamic State IS lomwe linakachitanso chiwembu ndi kupha anthu oposera zana limodzi mdziko la France la Boko Haram m’dziko la Nigeria ndinso la Al Shabaab m’dziko Somalia.
M’tsogoleri wa dziko la America a Barack Obama wati dziko la America liyesetsa pothana ndi magulu a zigawenga omwe akulimbikitsa ziwembu m’mayiko osiyanasiyana.
Iye walakhula izi pokhudzidwa ndi imfa ya anthu khumi ndi anayi omwe aphedwa pa chiwembu chomwe magulu ena a zauchifwamba achititira anthu okhala ku San Bernardino m’dzikomo.
Iye wati zomwe zachitikazi ndi zokhudza kwambiri choncho mkofunika kuti dziko lake litengepo mbali pa ntchito zowonetsetsa , kuti anthu a m’dzikomo akukhala mwa bata ndi mtendere.
Magulu a zigawenga omwe padakali pano ndi amene akusowetsa mtendere m’mayiko osiyanasiyana ndi monga la Islamic State IS lomwe linakachitanso chiwembu ndi kupha anthu oposera zana limodzi mdziko la France la Boko Haram m’dziko la Nigeria ndinso la Al Shabaab m’dziko Somalia.