Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Usi Wapempha Mutharika Asasainire Bilu ya Malo

$
0
0

Katswiri pankhani ya zisudzo m`dziko muno Michael Usi, wapempha mtsogoleri wadziko lino ProfessorArthurPeter Mutharika asasainile lamulo latsopano lokhudza malo kamba koti a Malawi ambiri kuphatikizapo mafumu sanafunsidwe maganizo. 

A Usi anena izi poyakhura ndi Radio Maria Malawi munzinda wa Blantyre.

Iwo ati boma komanso nyumba ya malamulo akuyenera  kuzindikiritsa anthu magawo omwe ali mu lamulori .

Nyumba ya malamulo yavomereza lamulo latsopano lokhudza malo posachedwapa lomwe kwambiri likupereka mphamvu zambiri kwa nduna ya zamalo kuti izitha kupanga chiganizo  pa malo omwe kale anali m`manja mwa mafumu.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>