Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Afa Atawombedwa ndi Mphenzi ku Dowa

$
0
0

Bambo wina wafa m’phenzi itamuomba m’boma la Dowa.

Malingana ndi wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo SergeantRichard Kaponda, bambo-yu ndi Dalitso Jose yemwe anali wa zaka 38zakubadwa ndipo amachokera m’mudzi mwa Gomam’dera la mfumu yayikulu Msakambewa m’bomalo .

SergeantKapondaati ngozi-yi inachitikira m’mudzi mwa Gunda m’bomalo.

Iwo ati adakalipano mwana wa malemu-wa Lustia amugonekanso pa chipatala china m’bomalo atakhudzidwanso ndi ngozi-yi pa tsikuli.

Ofalitsa nkhani za apolisiyu wati mphenzi-yi inaomba ndi kupha bambo-yu ali m’nyumba kubisala mvula yamphamvu yomwe imagwa ku delaro. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>