Anthu 13, 000 Aphedwa Pa Ndende Ya Saydnaya Mdziko La Syria
Anthu oposa 13, 000 ati ndi omwe aphedwa mwachinsinsi pa ndende ya Saydnaya mdziko la Syria. Malinga ndi lipoti lomwe bungwe la Amnesty International latulutsa, anthu akhala akuphedwa pa ndendeyi...
View ArticleECM Yasankha Bambo Likutcha Kukhala Mlangizi wa Apolisi
Bungwe la ma episkopi mdziko muno la Episcopal Conference Of Malawi [ECM] lasakha Bambo Steven Likhucha kukhala mlangizi wa apolisi mumpingowu m’dziko muno. Bungweli lanena izi kudzera muchikalata...
View ArticleDayosizi ya mangochi Ikhazikitsa Ntchito Yobzala Mitengo
Dayosizi ya mpingo wa katolika ya Mangochi yati ili ndi chidwi chofuna kubwezeretsa chilengedwe mchimake. Episkopi wa dayosiziyi Ambuye Montfort Stima ndi omwe anena izi pa mwambo omwe anawatsogolera...
View ArticlePapa Wati Anthu a Mdziko la Myanmar Akufunika Mapemphero
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha anthu kuti apemphelere anthu a mdera la Rohingya mdziko la Myanmar omwe akuphedwa komanso kukakamizidwa kuti achoke mnyumba zao....
View Articlekubisala mvula yamphamvu yomwe imagwa ku delaro. Dziko Silingasangalatse...
Mtsogoleri wa mpingo wa Katolika pa dziko lonse Papa Francisko wati popanda amayi dziko silingasangalatse konse. Iye amalankhula izi ku mwambo wa nsembe ya Misa ku Santa Marta mu mzinda wa Vatican....
View ArticleMOAM Ipempha Boma Liwunikenso Misonkho
Bungwe la eni minibus m`dziko muno la Minbus Owners Association of Malawi(MOAM) lapempha boma kuti liwunikenso misonkho pofuna kuti ikhale yokomera anthu ochita malonda ang’onoang’ono omwe ambiri...
View ArticleAfa Atawombedwa ndi Mphenzi ku Dowa
Bambo wina wafa m’phenzi itamuomba m’boma la Dowa. Malingana ndi wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo SergeantRichard Kaponda, bambo-yu ndi Dalitso Jose yemwe anali wa zaka 38zakubadwa ndipo amachokera...
View ArticleTrump Akulingalira Zosintha Pang’ono Lamulo Loletsa Mzika za Maiko a Chisilamu
Mtsogoleri wa dziko la America Donald Trump wati ali ndi malingaliro ongofuna kusintha pang’ono ganizo lake loletsa nzika za mayiko ena achisilamu kulowa mdzikolo. A Trump alengeza izi pomwe khoti lina...
View ArticleMOAM Ipempha Boma Liwunikenso Misonkho
Bungwe la eni minibus m`dziko muno la Minbus Owners Association of Malawi(MOAM) lapempha boma kuti liwunikenso misonkho pofuna kuti ikhale yokomera anthu ochita malonda ang’onoang’ono omwe ambiri...
View ArticleAnthu 7 Afa pa Chiwembu Mdziko la China
Anthu asanu ndi atatu afa ndipo ena asanu avulala potsatira chiwembu cha mipeni chomwe chinachitika mdera la Xinjiang mdziko la China. Mwa anthu omwe afawo ndi kuphatikizapo atatu omwe akuwaganizira...
View ArticlePapa Francisco Wapempha Akhristu Azikhala Okondwera mu Chikondi cha Mulungu.
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti azikhala okondwera nthawi zonse mu chikondi cha Mulungu. Papa amalankhula izi lero ku likulu la mpingowu ku Vatican...
View ArticleAchinyamata Azigwiritsa Bwino Ntchito Luso la Makono Pofalitsa Uthenga wa...
Achinyamata a bungwe la Young Christian Workers (YCW) mumpingo wa katolika awalangiza kuti azigwiritsa bwino ntchito maluso atsopano omwe akubwera mdziko muno monga ma computer komanso internet...
View ArticleAkatolika Mdziko La India Apempha Boma Litenge Gawo Mpaka Bambo Tom Apezeke
Akhristu a mpingo wakatolika mdziko la India apempha boma la dzikolo kuti likambirane ndi maiko a mchigawo chapakati chakuzambwe ndi cholinga choti atulutse bambo Tomomwe anagwidwa mdziko la Yemen ndi...
View ArticleKulowa ma Bungwe Awiri a Nkhonya ndi Kuphwanya Malamulo-MPBCB
Bungwe lalikulu loyang’anira akatswiri omenya nkhonya mdziko muno la Malawi Professional Boxing Control Board lati ndi lokhumudwa kaamba ka mchitidwe wa omenya nkhonya ena omwe akugwira ntchito ndi...
View ArticleArkidayosizi ya Blantyre Ipempha Akhristu Abwezeretse Chilengedwe
Arkidayosizi ya mpingo wa katolika ya Blantyre yalimbikitsa akhristu a mpingowu kuti abzale mitengo ngati njira imodzi yobwezeretsa chilengedwe mdziko muno. Vicar General wa arkidayosiziyi bambo...
View ArticleMwana Afa Atamira M’madzi M’boma la Mangochi
Mwana wina wa chaka chimodzi wafa atamira m’madzi m’boma la Mangochi. Izi zachitika m’mudzi mwa Chipoka mfumu yaikulu Mponda m’bomalo. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Inspector Rodrick Maida wauza...
View ArticleKuthetsa Matola Kwachepetsa Ngozi M’boma la Mangochi
Kuletsa kwa galimoto za matola m’boma la Mangochi ati kwathandiza kubweretsa bata pa nsewu komanso kuchepetsa ngozi za pansewu m’bomalo. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo inspector Rodrick Maida...
View ArticleBambo wina wadzipha Podzimangilira
Bambo wina wa zaka 49 zakubadwa wa mmudzi mwa Steven mdera la mfumu yaikulu Chowe m’boma la Mangochi wafa kaamba kodzimangilira mu mtengo. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Inspector Rodrick Maida...
View ArticleAnthu Omwe Akuthandizidwa ndi CADECOM Akhale Odziyimira Pawokha-Ambuye Stima
Episkopi wa dayosizi ya mpingo wa katolika ya Mangochi Ambuye Montfort Stima apempha anthu omwe akuthandizika ndi bungwe lowoona za chitukuko mu mpingowu la CADECOMkuti akhale odziyimira pawokha...
View ArticleMisa ya Mwezi ndi Mwezi Ikuthandiza Amayi a Katolika Kuzama pa Chikhristu
Amayi a mpingo wa katolika mu parishi ya Chisitu mu arkidayosizi ya Blantyre ati miyoyo yawo ya chikhristu ikuzama pomwe akumakhala ndi mwambo wa nsembe ya ukaristia mwezi ndi mwezi. Mkhalapampando wa...
View Article