Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Anthu 20 Afa Boti Litamira Mdziko la Myanmar

$
0
0

Anthumakumi awiri (20)afa boti lomwe anakwera litaombana ndi  linzake ndi kumira mu m’tsinje wina m’dziko la Myanmar.

Malingana ndi malipoti a News 24 anthu amene anali mu botili ndi oti anali akuchokera ku mwambo wa ukwati ku dela lina ndipo onse analipo 60.

Malipoti-wo ati mwa anthu omwe afawo 16ndi amayi ndipo anayiwo ndi amuna.

Ngozi za pamadzi akuti zimakonda kuchitikachitika mdzikomo kamba koti anthu ambri amakonda kugwilitsa ntchito maulendo a pamadzi.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>