Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Unduna Upempha Alimi Asagulitse Mbewu Mwachangu

$
0
0

Unduna wa zaulimi, ulimi wa m’thilira ndi chitukuko cha madzi wapempha alimi kuti ayambe kugulitsa mbewu zawo boma likakhazikitsa mitengo ya m’bewu-zo ya mbewuzo.

M’modzi mwa akulu-akulu mu unduna-wu a Steven Mbewe ndi omwe alankhula izi m’dera la mfumu yaikulu Njolomole m’boma la Ntcheu pa chionetsero cha ulimi-wa soya.

Polankhulapo m’modzi mwa akuluakulu ku bungwe lowona za chitukuko mu mpingo wakatolika mu dayosizi ya Dedza la CADECOM a Aaron Kalamule ati Iwo ngati bungwe sangawaletse alimi kugulitsa mbewu zawo koma akuyenera kupeza misika yomwe angathandize kuti apeze phindu lokwanira pa zokolora zawo.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>