Dziko la Yemen Lili pa Mavuto a Njala
Dziko la Yemen lapempha chithandizo kwa maiko akufuna kwabwino pamene likukumana ndi vuto la njala. Malipoti a wailesi ya BBC ati ngakhale dzikolo linali losauka ndi kale, nkhondo ya pachiweniweni...
View ArticleUnduna Upempha Alimi Asagulitse Mbewu Mwachangu
Unduna wa zaulimi, ulimi wa m’thilira ndi chitukuko cha madzi wapempha alimi kuti ayambe kugulitsa mbewu zawo boma likakhazikitsa mitengo ya m’bewu-zo ya mbewuzo. M’modzi mwa akulu-akulu mu unduna-wu a...
View ArticleMaternity Worldwide Ipereka Njinga 8 M’boma La Zomba
Bungwe la Maternity World Wide lapereka njinga za ambulance zokwana zisanu ndi zitatu 8 ku dera la gulupu Village Headman Kathebwe kudera la mfumu yaikulu Mwambo m’boma la Zomba. Bungweli lachita izi...
View ArticlePapa Ayamikira Akuluakulu a Papal Foundation
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wayamikira akuluakulu omwe amayendetsa bungwe la Papal Foundation kaamba ka ntchito yomwe akugwira. Papa wayamikira akulu-akulu-wa lero...
View ArticleMsungwana Afa Atagundidwa ndi Galimoto M’boma la Ntchisi
Msungwana wina wa zaka zisanu ndi chimodzi 6wafa atagudidwa ndi galimoto pa msika wa Khuwi m’boma la Ntchisi. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergeant Gladson M’bumpha watsimikiza za nkhaniyi...
View ArticleOphunzira a CHANCO Achita Ziwonetsero za Bata
Ophunzira ku sukulu ya ukachenjede ya Chancellor mu mzinda wa Zomba achita ziwonetsero za bata pomwe anakapeleka chikalata cha madandaulo awo kwa bwanamkubwa wa boma la Zomba chopempha m’tsogoleri wa...
View ArticleAtolankhani Awayamikira Kamba Kovumbulutsa Zinthu Zobisika
Atolankhani m’dziko muno awayamikira kamba kodzipereka pa ntchito zofalitsa mauthenga othandiza pa chitukuko cha miyoyo ya anthu m’dziko muno. Ena mwa anthu omwe athilira ndemanga pa za momwe ntchito...
View ArticleMpingo wa Anglican Ukusowa Thandizo la Ana Amasiye
Mpingo wa Anglican m’boma la Kasungu wapempha anthu akufuna kwabwino kuti athandize malo osamalirako ana amasiye ndi ovutika omwe mpingowu uli nawo ku Nthunthama m’bomalo. Mpingowu wati ukusowa...
View ArticleAmayi a Mpingo wa Katolika Ayenera Kusamalira a Mndende
Bungwe la amayi a mpingo wakatolika la Catholic Women Organisation (CWO)mu dayosizi ya Zomba lati amayi ali ndi udindo wosamalira anthu a m’ndende za mdziko muno. Mlembi wa bungweli mayi Catherine...
View ArticleMa Episkopi Adandaula Kamba ka Kusowa Kwa Ntchito
Bungwe la ma episikopi a mpingo wakatolika mchigawo cha m’mayiko a ku m’mwera kwa Africa la Southern Africa Catholic Bishops Conference, lati ndi lokhudzidwa ndi mavuto a kusowa kwa ntchito omwe...
View ArticlePapa Achita Chotheka Kuthetsa Nkhondo Mdziko la Venezuella
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wati achitapo kanthu pofuna kuthetsa nkhondo ya pachiweniweni yomwe ikuchitika mdziko la Venezuela. Papa amalankhula izi lamulungu pa bwalo...
View ArticleAnthu Awiri Afa pa Ngozi ya pa Msewu Mboma la Zomba
Anthu awiri afa ndipo ena 33 avulala m’boma la Zomba galimoto lomwe anakwera litagubuduzika pa malo ena otchedwa Chikupila m’bomalo. Malinga ndi wofalitsa nkhani za apolisi mchigawo chakuvuma...
View ArticleAkhristu Apemphelere Mtendere
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu a mpingowu kuti apempherere mtendere pa dziko lonse pansi. Malingana ndi malipoti a wayilesi ya Vatican Papa Francisco...
View ArticleAchinyamata Akhale ndi Mtima wa Utumiki
Achinyamata a mpingo wakatolika mdziko muno ati akuyenera kukhala ndi mtima wa utumiki komanso akhale okonda kupemphera. Episkopi wa dayosizi ya Mzuzu Ambuye John Ryan ndi omwe apereka pempholi ku St...
View ArticleApempha Boma Liwamangire ma Hostel
Ophunzira achitsikana pa sukulu ya sekondale yoyendera ya Changali m’dera la a Senior Chief Chimwala m’boma la Mangochi apempha boma kudzera mu unduna wa za maphunziro kuti uwamangire Hostel pa...
View ArticlePapa Francisco Ayendera Dziko la Portugal
Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wanyamuka kupita mdera la Fatima mdziko la Portugal komwe akakhale nawo pa chikondwelero chakuti padutsa zaka 100 chiwonekereni amayi Maria...
View ArticleArchdayosizi ya Lilongwe Ikhazikitsa Ntchito Yotolera Thandizo Lomangira...
Akhristu a mpingo wakatolika mu Archdayosizi ya Lilongwe awapempha kuti agwirane manja pa ntchito yomanga cathedral yatsopano mu Archdayosiziyo. Mkulu woona za chuma mu Archdayosiziyi bambo Gerald...
View ArticleChiwerengero cha Anthu Opezeka ndi Kachilombo ka HIV Chatsika Mdziko la Malawi
Bungwe la National Aids Commission NAC lati ndi lokondwa kamba koti chiwerengero cha anthu omwe ali ndi kachilombo koyambitsa matenda a Edzi ka HIV mdziko muno chikutsika. Mmodzi mwa akuluakulu ku...
View ArticleAkuba Aba ku Parishi ya Ntcheu
Anthu anayi omwe sakudziwika aba katundu osiyanasiyana ku parishi ya mpingo wa katolika ya Ntcheu mu dayosizi ya Dedza. Wofalitsa nkhani za apolisi m’boma la Ntcheu Sub-Inspector Hastings Chigalu...
View ArticleRadio Maria Yayamba Masiku Atatu Othamanga Mwakathithi ndi Amayi Maria
Radio Maria Malawi molumikizana wayilesi zina za Maria za pa dziko lonse lero zayamba ulendo wa masiku atatu wothamanga ndi amayi Maria mwa kathithi ndi cholinga chofuna kupeza thandizo la ndalama...
View Article