Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Papa Francisko Apemphelera Mwapadera Anthu Okhudzidwa ndi Chiwembu Mdziko la Turkey

$
0
0

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransiskolamulungu anachita mapemphero a padera opemphelera anthu onse omwe akhudzidwa ndi chiwembu cha mabomba chomwe chachitika ku m’mwera kwa dziko la Turkey.

Malipoti a wailesi ya Vatican ati mapemphero-wa anachitikira pa bwalo la tchalitchi lalikulu la St. Peter’s ku Rome pomwe amapemphelera anthu makumi asanu omwe afa ndipo ena ochuluka omwe avulala pa chiwembuchi.

Pa mapemphero-wa Papa ndi akhristu omwe anasonkhana pa bwaloli anapempheleranso mtendere m’dziko la Turkey. Malinga ndi malipoti gulu la zauchifwamba la Islamic State (IS)ndi lomwe lachita chiwembuchi.      


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>