Quantcast
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ntchito Yokhadzikitsa Bungwe La Kolona Ikuyenda Ku Zomba.

Ntchito yokhadzikitsa bungwe lolimbikitsa mapemphero a kolona m’maparishi osiyanasiyana akuti ikuyenda bwino mu dayosizi ya zomba.

Mkulu wa bungwe-li a Grasiano Mukunuwa ndi omwe anena izi polankhula ndi mtolankhani wathu. Iwo alankhula izi pomwe mamembala abungwe-li amalimbikitsa ntchito za bungwe-li ku magomero parish mu dayosiziyi.

Iwo ati ndi okondwa kuti ma parish ambiri apempha kale akuluakulu a bungweli kuti akakhadzikitsenso bungweli kamba koti likuthandiza kuzamitsa moyo wachikhristu pakati pa akhristu a mpingowu pokonda kupemphera kolona.

Bungwe la lokona  linayambira ku parish ya Thunga mu Arch dayosizi ya Blantyre mu mwezi wa November mchaka cha 2015  ndi a Graciano Mukunuwa layamba kukhala lachikoka pakati pa akhristu ambiri a mpingo wakatolika m’dziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>