Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Achinyamata Awapempha Kukhala Omasuka Pofotokoza Nkhawa Zawo.

$
0
0

Mpingo wakatolika m‘dziko muno wapempha achinyamata kuti azikhala omasuka pofotokozera mpingo, pa zamavuto omwe amakhala akukomana nawo.

Mlembi wa mkulu , ku likulu , la mpingo wakatolika mdziko muno, ku Episicopal Comference Of Malawi (ECM) , bambo Henery Saindi, ndi omwe anena izi pakutha pa msonkhano wa achinyamata ndi nthumwi zochokera ku bungwe la Amecea umene umachitikira mu mdzinda wa Lilongwe ndipo m’mawu awo ati achinyamata akuyenera kukhala omasuka makamaka pa nkhani zokhuzana ndichipembedzo kuti azikhala ndi moyo wamphamvu pa chikhristu chawo.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>