Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Bungwe La Mayi Khanda Likufuna Kufikira Amalawi Onse M’dziko Muno

$
0
0

Bungwe lolimbikitsa nkhani za uchembere wabwino la  Mai Khanda Trust lati lili ndi mapulani ofuna kukuza ntchito zake m’dziko muno.

Mkulu woona ntchito za m’bungwe-li a Edward Moses ndi amene wanena izi polankhula ndi mtolankhani wathu amene amafuna kudziwa zambiri zokhudza bungweli.

A Moses ati padakalipano bungweli likugwira ntchito zake m’maboma ena a m’chigawo cha pakati  koma liyetsetsa kuti ntchitozi zifalilkire m’dzigawo zonse m’dziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>