Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ansembe Sakuloledwa Kutsogolera Miyambo ya Maliro ya Anthu Odzipha

$
0
0

Mpingo wakatolika m’dziko la CANADA wati ansembe ampingowu sakuloledwa kutsogolera miyambo ya maliro aanthu amene amwalira mwakufuna kwawo.

Ma-episikopi a mpingo-wu anena izi kudzera mu uthenga wawo. Iwo alankhula izi potsatira kuvomelezedwa kwa lamulo lomwe likupeleka mwayi anthu woti amwalire n gati afuna kutero pa zifukwa zawo.

Pothililapo ndemanga pa nkhaniyi m’modzi mwa ma episcope-wa Arch-Bishop Richard Smith wa arch-dayosizi ya Edmonton wati chiphunzitso cha mpingo sichimavomeleza imfa za mdundu-wu chifukwa ndi imfa zomwe zimadza mosemphana ndi chifuniro cha mulungu.

Iye wati kudzipha ndi m’chitidwe wothandizira imfa ya munthu wina kapena kudzipha kumene ndi zosayenera pamaso pa Mulungu.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>