Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Anthu Agwilitse Ntchito Bwino Zinthu Zomwe ali Nazo-ECM

Bungwe la ma episikopia mpingo wakatolika m’dziko muno la Episcopal Conference of Malawi (ECM) lati anthu m’dziko muno angachite bwino pa chitukuko cha miyoyo yawo ngati angachilimike pogwilitsa bwino...

View Article


Bambo Chingale Asankhidwa Kukhala A Vicar Genenal A Dayosizi Ya Mangochi.

Episikopi wa mpingo wakatolika mu dayosizi ya Mangochi olemekezeka Ambuye Montfort Stima wasankha bambo Frank Chingale kukhala Vicar General wa dayosizi-yi kuyambira pa 30 August 2017. Padakalipano...

View Article


Zotsatira Za Mayeso A Junior Certificate Zatuluka.

Zotsatira za mayeso a Junior Certificate omwe ophunzira a form 2  analemba m’dziko muno  akuti zatuluka. Bungwe la New Independent Academic Examination Council ndi lomwe linagwira ntchito yolembetsa...

View Article

Msonkhano wa bungwe la CWO Mu Dayosizi Ya Zomba

Msonkhano wa amayi a wakatolika mu dayosizi ya zomba wayamba pa 31 August 2017 ndipo udzatha pa  3 September 2017. Polankhula potsekulira msonkhano-wu Episikopi wa mpingo wakatolika mu dayosizi-yi...

View Article

Apempha Mabungwe Kuti Azigwira Ntchito Limodzi Polimbana Ndi Matenda A Edzi

Bungwe la National Aids Commission (NAC) lapempha mabungwe omwe siya a a boma omwe akugwira ntchito zolimbana ndi matenda a edzi m’boma la Zomba kuti azigwira ntchitozawo limodzi ndi a ku khonsolo,...

View Article


Anthu 21 Afa Nyumba Itawagwera Mu M’dzinda Wa Mumbai M’dziko La India.

Anthu 21 afa nyumba ina yosanjikizana itawagwera mu m’dzinda wa mumbai m’dziko la India. Malingana ndi malipoti a BBC ambiri mwa anthu omwe afa pa ngozi-yi ndi omwe anali mkati mwa nyumbayi imene inali...

View Article

Mariatona wa Lokolo Atsekulidwa pa 15 October

Mwambo wotsekulira Mariatona wa lokolo akuti udzachitika loweruka pa 15 mwezi uno ku likulu kwa Radio Maria Malawi ku Mangochi. M’modzi mwa akulu akulu oyendetsa ntchito za Radio Maria Malawi a...

View Article

Ansembe Sakuloledwa Kutsogolera Miyambo ya Maliro ya Anthu Odzipha

Mpingo wakatolika m’dziko la CANADA wati ansembe ampingowu sakuloledwa kutsogolera miyambo ya maliro aanthu amene amwalira mwakufuna kwawo. Ma-episikopi a mpingo-wu anena izi kudzera mu uthenga wawo....

View Article


Station ya Sitima ya Nkaya Itha mu November

Gawo lachiwiri lomanga station ya sitima za pamtunda ya NKAYA m’boma la BALAKA akuti ikuyembekezeka kutha mwezi wa NOVEMBER chaka chino. Wofalitsa nkhani ku bungwe loona za sitima za pamtunda la...

View Article


Ambuye Tamba Awonetsa Chidwi Chothandiza Radio Maria Malawi.

Episikopi wa mpingo wakatolika mu dayosizi ya Zomba olemekezeka Ambuye George Desmond Tambala alimbikitsa ansembe mu dayosiziyo kuti apitirilize kuthandiza Radio Maria Malawi. Ambuye Tambala anena izi...

View Article

Awapempha Kuti Asamaope Kukhala M’maudindo Osiyanasiyana

Akhristu a mpingo wakatolika m’dziko muno awapempha kuti asamaope kukhala m’maudindo osiyanasiyana kamba koti kudzera m’maudindowa pomwe angathandize pa chitukuko cha dziko lino. Bambo Hennery...

View Article

Mariatona wa Lokolo Atsekulidwa pa 15 October

Mwambo wotsekulira Mariatona wa lokolo akuti udzachitika loweruka pa 15 mwezi uno ku likulu kwa Radio Maria Malawi ku Mangochi. M’modzi mwa akulu akulu oyendetsa ntchito za Radio Maria Malawi a...

View Article

Bambo Wina Amulamula Kukagwira Ukayidi Kwa Zaka 10 Pa Mulandu Wogwilira.

Bwalo loyamba lamilandu m’boma la Mwanza lalamula mwamuna wina wa zaka 28 zakubadwa kuti akakhale kundende kwa zaka 10 kaamba kopezeka olakwa pa mulandu wogwililira mwana wa msungwana wa zaka 15...

View Article


Amangidwa Kamba Kopezeka Ndi Ndalama Zachinyengo.

Apolisi ku Lumbadzi m’boma la Dowa akusunga m’chitolokosi bambo wina wa zaka 22 zakubadwa kamba kopezeka ndi ndalama zachinyengo. Malingana ndi wachiwiri kwa wofalitsa nkhani za polisi ku kanengo mu...

View Article

Bambo Willem Wester Amwalira

A Kulikulu la mpingo wakatolika m’dziko muno ku EPISCOPAL CONFERENCE OF MALAWI (ECM) alengeza za imfa ya bambo WILLEM WESTER omwe akhala akutumikira mpingowu ku ARCH DAYOSIZI ya Blantyre Bambo Wellem...

View Article


Ayamikira Anthu Chifukwa Chopereka Magazi

Bungwe lopereka magazi la MALAWI BLOOD TRANSFUNSION SERVICE (MBTS) layamikira anthu  a m’boma la Ntcheu kaamba kodzipereka pantchito yopereka magazi pamene bungweli limagwira ntchito yotolera magazi...

View Article

Akhiristu Apita Kumalo Oyera Ku Kibeho Mdziko La Rwanda

Akhristu amene  ali pa ulendo wa ku malo oyeraa KIBEHO m’dziko la RWANDA awapemphaakuti asadere nkhawa pa zaulendowu kaamba koti zomwe achitazi ndi zopambana mu mbiri ya moyo wawo wa chikhristu. Izi...

View Article


Papa Alimbikitsa Ubale wa Pakati pa Mpingo Wakatolika ndi Anglican

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu a mpingo wa katolika ndi Anglican kuti azigwilira ntchito limodzi ndi cholinga chofuna kulimbikitsa umodzi pakati pawo....

View Article

Anthu Asanu ndi Ena Atatu Afa pa Ngozi ya Pansewu

Anthu asanu ndi ena atatu (8) afa ndipo ena avulala modetsa nkhawa mini-bus yomwe anakwera itagubuduzika ku Nguludim’boma  la Chiladzulu. Malinga ndi m’modzi mwa  omwe apulumuka pa ngoziyo mai Annie...

View Article

Apempha Akhristu Kudzipereka Pofalitsa Uthenga Wa Mulungu

Kudzipereka pa ntchito yakufalitsa uthenga wa Mulungu akuti ndi njira yokhayo  imene imaonetsa chikhristu chenicheni. Abusa Joseph Maganga a mpingo wa CCAP  kuchokera ku Chiradzulu ndi omwe anena izi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>