Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Mayi Kajawo Ati ndi okondwa ndi thandizzo la M’thenda Ya Mtima Lomwe Mwana Walandira Mdziko La Italy

$
0
0

Makolo a m’sungwana yemwe wakhala akuvutika ndi mthenda ya mtima ati ndiokondwa kaamba ka thandizo lamphamvu lomwe mwana wawo walandira mdziko la Italy.

Polankhula ndi Radio Maria Malawi Mai Catherine kajawo anathokoza bambo Josephy kimu omwe ndi a Director a Radio Maria Malawi pa thandizo lomwe anawachitira powapezera njira yabwino yokapezera thandizoli mdziko laItaly.

Mai Kajawo anati pa Iwo okha sangathe kuthokoza koma Mulungu yekha ndi yemwe angathe kubweza madalitsowo.

Ndipo pothokoza mulungu nsungwana yemwe wakhala akudwalayu Regina Kajawo anati pano ndiokondwa kaamba koti akutha kupanga chilichonse kusiyana ndi kale.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>