Quantcast
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ambuye Msusa Apepesa Amayi kamba ka Nkhanza Zomwe Akukomana Nazo.

Arch-Dayosizi ya mpingo wakatolika ya Blantyre yati ndiyokhudzidwa kwambiri ndi nkhanza zomwe zikupitilira kuchitika pakati pa amayi m’dziko muno.

Arch-Episikopi wa mpingowu mu Arch-Dayosizi-yi , Ambuye Thomas Luke Msusa , ndi amene wanena izi pa mwambo wa msembe ya ukaristia yokondwelera chaka cha umayi wa a mayi Maria, yomwe inakonzedwa ndi bungwe la amayi a chikatolika la Catholic Women Organisation mu Arch Dayosizi-yi.

Chaka cha umayi wa amayi maria cha mu arch dayosizi ya Blantyre chinachitikira kwa Mwanga Parish.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>