Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Papa Wati Akhristu Kuyenera Kukahala Achikondi Ndi Olimba Pa Chikhulupiliro

$
0
0

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse papa Francisco wapempha akhristu kuti azikhala achikondi ndi olimba pa chikhulupiliro chawo.

Papa walankhula izi pomwe amathililapo ndemanga pa zakutchulidwa kwa akhristu 35 a mpingo-wu kuti ndi oyera.

akhristu-wa avomelezedwa pa 15 october ndi mpingo-wu kuti ndi oyera mu mpingo, pa mwambo waukulu , umene unachitikira pa bwalo La St Peters Square , ku likulu la mpingo-wu ku Vatican.

Oyera atsopano mu mpingowu , achokera m’mayiko a Brazil,  Mexico, Spain ndinso Italy.  mwa oyera atsopano-wa muli amsembe awiri.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>