Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ayamikira Atolankhani Pa Nkhani Yofalitsa Mauthenga a Nkani Zokhuzana ndi Kupopa Magazi.

$
0
0

Bungwe lomenyera ufulu wa atolankhani m’dziko muno la Media Institute Of Southern Africa (Misa-Malawi)  layamikira atolankhani momwe akugwilira ntchito zawo pofalitsa mauthenga okhudza mpheketsera yokhudzana ndi nkhani zopopa magazi zomwe zakhala zikumveka m’mamboma ena m’dziko muno.

Wapampando wa bungwe-li a Tereza Ndanga , ndi amene wanena izi polankhula ndi mtolankhani wathu amene amafuna kumva ndemanga za bungweli , pa za momwe atolankhani agwilira ntchito zawo pofalitsa nkhani zokhudza mpheketsela ya zopopa magazi-yi m’dziko muno. Ndanga wati bungwe la Misa kuno ku Malawi liyesetsa kupeleka ukadaulo woyenera wofalitsira nkhanizi kwa atolankhani m’dziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>