Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Apempha Boma Kusintha Zina Mwandondomeko Zake Zoyendetsera Dziko.

$
0
0

chipani cholamula cha Democratic Progressive(DPP), kuti chikonze mavuto omwe anthu akukumana nawo m’dziko muno.

Polankhula ndi Radio Maria Malawi mu m’dzinda wa Blantyre a Hamphrey’s Mvula ati chipani chomwe chimakhala chikulamula m’dziko, chimayenera kumakwanilitsa kutumikira anthu pa zosowa zawo nthawi zonse. Iwo anena izi potsatira kusachita bwino kwa chipani cholamula cha Democratic Progressive (DPP) pa chisankho chachibwereza chomwe chinachitika pa 17 October, 2017 m’madera ena a dziko lino.

M’mawu awo a Mvula atinso nthawi yakwana yoti anthu azikhala ndi nthawi yopanga maganizo azofuna zawo mwaufulu posatengera kusiyana kwa zipani ndipo apemphanso chipani chalamula mdziko muno kuti tsopano ndi nthawi yoti akonze zina mwa njira zomwe zapangitsa kuti chisachite bwino pa chisankho cha chibweleza chomwe chinachitika masiku apitawa.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>