Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Kuchuluka Kwa Zipani Kulibe Vuto, Koma...

$
0
0

Mtsogoleri wa chipani chotsutsa boma cha Umodzi, Professor John Chisi wati sakuwonapo vuto pa kuchulukana kwa zipani za ndale mdziko muno.

Professor Chisi wanena izi polankhula ndi Radio Maria Malawi. Iye wati ngakhale dziko lino litakhala ndi zipani mazanamazana koma chofunika kwambiri ndi choti zipanizo zibweretse mgwirizano pakati  pa a Malawi mdziko muno.

Ndipo polankhulapo, m’modzi mwa ankhlakale pa ndale mdziko muno a Humphreys Mvula agwirizana ndi a Chisi pa nkhaniyi koma ati kuchuluka kwa zipani kumasokoneza ntchito za chitukuko mdziko.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>