Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Papa Francisco wakhuzidwa ndi za chiwembu zomwe zachitika mdziko la France.

$
0
0

M’tsogoleri wa mpingo wa Katolika pa dziko lonse Papa Francisco  wati ndi wokhudzidwa ndi imfa ya atolankhani a ku kampani ina yolemba nkhani omwe aphedwa lachitatu mu mzinda wa Paris  m’dziko la France.

Mu uthenga omwe likulu lampingowu ku Vatican latulutsa, Papa wati  imfa ya anthuwa, omwe anachita kuwombeledwa ndi anthu ena osadziwika ,yasokoneza mtendere m’dziko la France .

Padakalipano apolisi mdzikolo akuti agwira  anthu asanu ndi awiri powaganizira kuti akukhudzidwa ndi imfa ya atolankhaniwo.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko