Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Bungwe la PMS Layamikira Makolo ndi Atsogoleri a Mpingo Pokometsa Utumiki wa Ana

Mkulu woyan’ganira mabungwe a utumiki wa a Papa m’dziko muno,  wayamikira makolo ndi atsogoleri a mpingo  chifukwa chothandiza kukometsa chaka cha  utumiki wa ana  chomwe chachitika  lamulungu la...

View Article


Akhristu Adzipereke Popititsa Patsogolo Moyo wa Miphakati

Akhristu a mparish ya St Martin Chirimba mu Archdayosizi ya Blantyre awapempha kuti adzipereke popititsa patsogolo moyo wa miphakati mparishiyi. A Robert Msakambewa omwe ndi wapampando wa Parishiyi...

View Article


Episkopi wa Dayosizi ya Mangochi Walimbikitsa Akhristu a ku Mvunguti kuti...

Episkopi wa dayosizi ya Mangochi Ambuye Montfort Sitima, alimbikitsa akhristu aku Mvunguti mparishi ya Nankhwali mudayosiziyi,kuti asafowoke pa chikhristu chawo ngakhale akukumana ndi mavuto...

View Article

Akhristu Akuyenera Kukometsa Moyo Wawo wa Uzimu mu Chaka Chatsopanochi

Akhristu a mpingo wa katolika awapempha kuti pamene chaka chatsopano chayamba ayambiretu kutekeseka mu njira zosiyanasiyana pofuna kukometsa moyo wawo wauzimu. Wansembe owona za utumiki mu Archdayosizi...

View Article

Wapampando wa Bungwe la AMECEA Asankhidwa Kukhala Kadinala

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francis, wakweza paudindo wampando wa  bungwe la maepiskopi a mdera kumvuma kwa Africa la AMECEA olemekezeka Ambuye Berhaneyesus Demerew Souraphiel...

View Article


Episkopi wa Dayosizi ya Mangochi Wathokoza Akhristu Podzipereka mu Chaka Chatha

Episkopi wa Dayosizi ya Mangochi Ambuye Montfort Stima wayamikira akhristu a mpingowu mu Dayosiziyi kamba kodzipeleka pothandiza mpingo mu njira zosiyanasiyana m’chaka changothachi. Ambuye Stima...

View Article

Akhristu ndi Anthu Akufuna Kwabwino Apitirize Kuthandiza Radio Maria Malawi

Akhristu ndi anthu ena akufuna kwabwino m`dziko muno awapempha kuti athandize Radio Maria Malawi mu nyengo ino kuti ithe kupitiliza kutumikira anthu moyenera. Wapampando wa Parish ya Mzedi mu...

View Article

Dziko la Canada Lakhazikitsa Lamulo Lolemekeza Malemu Papa Yohane Paulo...

Nyumba ya malamulo mdziko la Canada yakhadzikitsa tsiku lachiwiri m’mwezi wa April chaka chilichonse kuti anthu mdzikolo, adzikumbulira mtsogoleri wakale wa mpingo wakatolika  malemu Papa Yohane Paulo...

View Article


Zokonzekera Mwambo wa Chikondwelero cha Kachebere Seminale Zikuyenda Bwino

Zokonzekera  mwambo otsekulira chikondwelero chakuti  sukulu yosulira ansembe ya Kachebere m’boma la Mchinji yatha zaka 75 chiyambire ntchito zake akuti zikuyenda bwino. Wapampando wa komiti yomwe...

View Article


Makhansala Apempha Boma kuti Liwapatse Ngongole

Bungwe la makhansala mdziko muno la Malawi Local Government Association (MALGA), lapempha boma kuti lipereke ngongole yogulira njinga za moto yomwe lidalonjeza kuti lipereka kwa makhansala  pofuna kuti...

View Article

Kubadwa kwa yesu

Kubadwa kwa yesu Montfort Media Matamando choir mangochi diocese

View Article

Angero adika

Angero adika Kaggwa woyera Choir 1 Lilongwe Archdiocese

View Article

Lamulo lidatuluka

Lamulo lidatuluka by Mangochi Cathedral

View Article


Tikondwere tiimbe

Tikondwere tiimbe by All Saints Likuni Choir Lilongwe Archdiocese

View Article

Anjero adika

Anjero adika by St Maseline choir domasi college zomba diocese

View Article


Ambuye wabadwa

Ambuye wabadwa by St Tereza Chikalimbo choir Magomero Parish Zomba Diocese

View Article

Tikondwerera

Tikondwerera by St Francisco bossache njale parish Bt Archdiocese

View Article


Papa Francisco wakhuzidwa ndi za chiwembu zomwe zachitika mdziko la France.

M’tsogoleri wa mpingo wa Katolika pa dziko lonse Papa Francisco  wati ndi wokhudzidwa ndi imfa ya atolankhani a ku kampani ina yolemba nkhani omwe aphedwa lachitatu mu mzinda wa Paris  m’dziko la...

View Article

Mchitidwe Wozembetsa Anthu Akuti Ukupitilirabe M`boma la Mangochi

Bungwe la Rights Advice Center m’boma la Mangochi lati lakonza mapulani omwe athandize kuthana ndi m’chitidwe wozembetsa anthu m’bomalo. Mkulu wa bungweli m’bomalo a Madalitso Masache ndi yemwe wanena...

View Article

Madzi Apha Munthu M`modzi Ndikuvulaza ena Atatu M`boma la Zomba.

Munthu m’modzi wafa ndipo ena atatu akuti  avulala ndi madzi osefukira mu m’tsinje wa Likangala  m’boma la Zomba. Malinga ndi Wofalitsa nkhani za apolisi m`boma la Zomba  Constable Patricio Supliano...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>