Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Mabungwe omwe si Aboma Achita Ziwonetsero

$
0
0

Ziwonetsero zofuna kukakamiza mabungwe omwe analandira thandizo la ndalama  kuchokera ku bungwe lowona za matenda a Edzi mdziko muno la National Aids Commission  NAC kuti abweze ndalamazi zachitika lachiwiri mmizinda yonse mdziko muno.

Paziwonetserozi mabungwe omenyerera Ufulu wa anthu mdziko muno,apereka chikalata chamadandaulo awo pa nkhaniyi.

Kudzera mchikalatachi,mabungwewa awopseza kuti ngati mabungwe omwe analandira thandizoli kuchokera kubungwe la NAC sabweza ndalamazi pasanathe masiku 100, achita zinthu zomwe chikalatacho sichidanene.

 

 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>