Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Mwambo Wansembe Ya Ukalistia Opemphelera Akhristu Opita ku Yerusalemu Wachitika Dzulo.

$
0
0

Mwambo wa Nsembe ya Ukaristia opemphelera ulendo okayendera malo oyera mdziko la Israel wachitika lachitatu ku Parish ya St Patricks mu Arkdayosizi ya Lilongwe.

 Akhristu oposa makumi anayi ndiwomwe akupita kuulendowu ndipo ena mwaiwo  ndi Ansembe anayi ndi Sisiteri mmodzi.

Akhristuwa akuyembekezeka kukayendera ndi kupemphera mmalo osiyanasiyana oyera kuphatikizapo pamanda pomwe Yesu Khristu adayikidwa ndi kuuka kwa akufa.

Akhristuwa akuyembekezeka kufika mdziko muno lachiwiri pa 23 June.

Chaka ndi chaka akhristu amapita ku Malo oyera ku Yeruselemu motsogozedwa ndi Bambo Joseph Kimu womwenso ndi mkulu woyanganila  Radio Maria Malawi mdziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>