Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

BUNGWE LA RED CROSS LAYAMBITSA NTCHITO YOLIMBIKITSA UCHEMBERE WABWINO

$
0
0

 

Bungwe la Malawi Red Cross layambitsa ntchito yolimbikitsa uchembere wabwino m’maboma a Kasungu ndi Ntchisi.

Ntchitoyi yomwe ndi ya ndalama zokwana 600 million kwacha ikuyembekezeka kuthandiza kuchepetsa imfa za amayi oyembekezera komanso ana m’mabomawo.

Ntchitoyi igwilidwa ndi thandizo lochokera ku boma la dziko la Belgia, ndipo ikuyembekezera kutha mwezi wa December.

Mkulu wa pa chipatala cha  Kasungu  Dr.Jeromy Nkambule athokoza bungweli kaamba kothandiza pa ntchito yolimbikitsa ntchito za uchembere wabwino m’mabomawo.

 

 

 

 

 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>