Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

PAPA FRANCIS AYAMIKIRA NYUMBA ZOFALITSA NKHANI

$
0
0

 

Mtsogoleri wa Mpingo wa Katolika pa dziko lonse lapansi Papa Francis wayamikira nyumba zofalitsa nkhani pa dziko lonse kaamba kotsatira ndi kulengeza bwino zonse zomwe zimachitika  ku likulu la Mpingowu kuchokera pomwe Papa opuma Benedikito wachi 16 atalengeza zopuma paudindowu mwezi watha.

Papa Francis amankhula izi ndi atolankhula ku likulu la mpingowu ku Vatican m'dzikolo.

Iye wati  nyumba zofalitsa nkhani zili ndi udindo ofotokozera anthu zinthu zosiyanasiyana kuphatikizapo za mu Mpingo.

Papa Francis walowa m’malo mwa Papa  Benedikito wa chi 16 yemwe adapuma pa udindowu mwezi watha mwa zina kamba koti wakula.

 

 

 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>