Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

MWAMUNA ADZIPHA PODZIMANGILIRA ATAKANGANA NDI MKAZI WAKE

Bozyolo  Chigwenembe wa zaka  22  zakubadwa wadzipha podzimangilira  pambuyo pokangana ndi  mkazi wake kwa mfumu yaikulu Dzoole m’boma la Dowa. Mneneli wa apolisi ku Mponela  m'bomalo a Kondwani...

View Article


MSONKHANO OYAMBA OKHUDZA KUSANKHA PAPA WATSOPANO

 Likulu la Mpingo wa Katolika ku Vatikani lalengeza kuti msonkhano oyamba wa makadinala okonzekerakusankha Papa watsopano uchitika pa 4 March 2013. Malinga ndi Chikalata chomwe mkulu wa makadinala omwe...

View Article


BAMBO HENLY CHAONA ALOWA M'MANDA LERO

  Mwambo woyika m’manda thupi la Malemu Bambo Henry Chaona  omwe adamwalira pa 2 March kuchipatala cha Malamulo mu mzinda wa Blantyre  uchitika pa 4 March 2013. Likulu la diocese ya Zomba ndi lomwe...

View Article

PAGOLOGOTA

Lent track titled Pagologota by ST Peters Choir Doviko Church Tsangano Parish

View Article

DEMOKALASE KAPENA DEMONI KALASI?

Ulaliki titled Demokalase kapena Demoni Kalasi? by Father Mwinganyama

View Article


MBUYE YESU NDI ZINGWE ZIJA

Lent track titled Mbuye Yesu ndi Zingwe Zinja by ST Simon and Jude Catholic Choir

View Article

ASEMINO 55 A CHAKA CHOYAMBA ALANDIRA MIKANJO

  Asemino 55 ochokera m’madayosizi  asanu ndi atatu  a Mpingo wa Katolika m'dziko muno alandira mikanjo  ku sukulu yosula ansembe ya Kachebere ku Mchinji mu arkidiocese ya Lilongwe. Episkopi wa...

View Article

ALIYENSE ABWERE NDI CHACHIKHUMI KUNYUMBA KWANGA

Ulaliki titled Aliyense Abwere ndi Chachikhumi  Kunyumba Kwanga by Father Nthalika

View Article


INE NDI NTCHITO ,NDI MCHERE WA ANA

Ulaliki titled Ine Ndi Ntchito, ndi Mchere wa Ana

View Article


GWIRITSANI NTCHITO NDALAMA

Ulaliki titled Gwiritsani Ntchito Ndalama by Father Nthalika

View Article

MWAMBO OSANKHA PAPA WATSOPANO ULI M'KATI

  Makadinala a Mpingo wa Katolika akupitiliza mwambo osankha Papa watsopano atalephera kupeza yemwe wapambana pachisankho chawo pa 12 March 2013.   Makadinala 115  ndiomwe akusankha Papa yemwe alowe...

View Article

KODI MPHAMVU ZANU MUMAZITENGA KUTI?

Ulaliki titled Kodi Mphamvu Zanu Mumazitenga Kuti? by Father Kimu

View Article

PAPA FRANSIS SAGWIRIZANA NDI MAUKWATI AMUNA KAPENA AKAZI OKHAOKHA

  Malipoti a catholic World News ati ngakhale kuti mtsogoleri wa mpingo wakatolika Papa Fransis ali omasuka  mu zambiri, sakugwizana kwambiri ndi  maukwati a pakati pa amuna kapena akazi okhaokha....

View Article


MPINGO WA KATOLIKA ULI NDI PAPA WATSOPANO

  Kadinala George Mario Bergolio wa m’dziko la Argentina ndiye mtsogoleri watsopano wa Mpingo wa Katolika pa dziko lonse lapansi. Kadinalayu wasankhidwa pa 13 March 2013 patangotha tsiku limodzi...

View Article

BOMA LICHITEPO KANTHU PANKHANI YOKWEZA MAPHUNZIRO

  Mpingo wa Katolika wati ukufunitsitsa kuti boma la Malawi liwunikenso bwino njira zomwe zidakhazikitsidwa poyendetsa ntchito zamaphunziro pofuna kuti  maphunziro apite patsogolo m’dziko muno. Mkulu...

View Article


PAPA FRANSIS ALIMBIKITSA CHIKONDI PAKATI PA OSAUKA-JAKAYA KIKWETE

  Mtsogoleri wa dziko la Tanzania a Jakaya Kikwete ati kusankhidwa kwa Papa Fransis kuthandiza kwambiri kupititsa patsogolo chikhulupiliro pakati pa a Katolika komanso anthu onse kaamba koti moyo wa...

View Article

A VUWA KAUNDA AMANGIDWASO POMWE AMAFUNA KUPITA KU ULAYA

 M'modzi wa akuluakulu a chipani cha Democratic Progressive DPP a Symon Vuwa Kaunda omwe anatulutsidwa pa belo sabata yangothayi awamanganso pa 17 March 2013 pomwe amafuna kukwera ndege kupita ku...

View Article


ANTHU 5 500 AFA NDI MATENDA A MALUNGO CHAKA CHATHA

Unduna wa za umoyo wati anthu 5 miliyoni ndi omwe anadwala matenda a malungo chaka chatha ndipo mwa anthuwa 5 Sauzande 5 handirede  adamwalira ndi matendawa ngakhale kuti matendawa ndi opeweka komanso...

View Article

PAPA FRANCIS AYAMIKIRA NYUMBA ZOFALITSA NKHANI

  Mtsogoleri wa Mpingo wa Katolika pa dziko lonse lapansi Papa Francis wayamikira nyumba zofalitsa nkhani pa dziko lonse kaamba kotsatira ndi kulengeza bwino zonse zomwe zimachitika  ku likulu la...

View Article

BUNGWE LA RED CROSS LAYAMBITSA NTCHITO YOLIMBIKITSA UCHEMBERE WABWINO

  Bungwe la Malawi Red Cross layambitsa ntchito yolimbikitsa uchembere wabwino m’maboma a Kasungu ndi Ntchisi. Ntchitoyi yomwe ndi ya ndalama zokwana 600 million kwacha ikuyembekezeka kuthandiza...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>