Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Apolisi Mdziko la Egypt Apha Anthu Khumi ndi Awiri

$
0
0

Apolisi mdziko la Egypt apha mwa ngozi anthu khumi ndi awiri kuphatikizapo nzika ya mdziko la Mexico yomwe imakayenda mdzikolo.

 

Anthuwo amayenda mugalimoto zinayi zomwe zinalowa kumalo ena otetezedwa.

 

Malipoti a wailesi ya BBC ati  anthu okwana khumi ochokera mdziko la Mexico ndi la Egypt anavulazidwanso ndipo akulandira thandizo ku chipatala cha boma mdzikolo.

 

Mtsogoleri wa dziko la Mexico a Enrique Pena Nietowati ndi okhudzidwa ndi nkhaniyi ndipo wati akufuna kuti  pakhale  kafukufuku wamphamvu ndi boma la Egypt.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>