Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Dziko la Swaziland Likufunika Mwambo wa Mapemphero

Episkopi  wa dziko la Swaziland  wapempha anthu m’dzikolo kuti akhale ndi mwambo wa mapemphero  potsatira ngozi ya pansewu  yomwe inapha  atsikana pafupifupi makumi asanu omwe adali paulendo...

View Article


Papa Francisco Wapepesa Anthu omwe Akhudzidwa ndi Mphepo ya Mkuntho

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco watumiza uthenga wa chipepeso kwa abale a anthu omwe akhudzidwa ndi mphepo ya mkuntho yomwe yachitika  pa doko la Caribean .   Mu uthengawo...

View Article


Bungwe la Mabanja Likondwelera Zaka 30 Chilikhazikitsire

Bungwe la mabanja mumpingo wa katolika m`dziko muno  ati lichita chaka chokondwerela kuti latha zaka makumi atatu chilikhazikitsire m`dziko muno. Banja lomwe likutsogolera bungweli a Godfrey ndi a...

View Article

Matupi a Asilikali Khumi a Mdziko la Uganda Apita Nawo Kwawo

Matupi khumi a asilikali a dziko la Uganda omwe anafa, gulu la zauchifwamba la Al-shabab litachita zamtopola kumalo omwe asilikaliwa amakhaka omwe ali pamtunda wamakilomita 90 kumm’wera chakunzambwe...

View Article

Pulezidenti wa Dziko la Guatemala Watula Pansi Udindo

Mtsogoleri wa dziko la Guatemala   a Perezi Molina watula pansi udindo wake komanso amangidwa kamba komuganizira kuti amachita zakatangale.   Malinga ndi  malipoti a wailesi ya Vatican  Pulezidenti...

View Article


Chipani cha SBVM Chikondwelera Zaka 90 Chikhazikitsire

Asisteri a Chipani cha atumiki a maria virgo woyera Sisters of the Blessed Virgin Mary SBVM mu mpingo wakatolika awayamikira kamba ka ntchito zosiyanasiyana zomwe akhala akugwia m’dziko muno....

View Article

Matupi a Anthu 61 omwe Anafa pa Ngozi ya Bwato Mdziko la Malaysia Apezeka

Matupi a anthu 61 a mdziko la Indonesia omwe anafa pa ngozi ya  bwato  lomwe anakwera litamila lachinayi sabata yatha mdziko la Malaysia, apezeka lolemba. Malinga ndi malipoti a nyuzi 24 anthuwo...

View Article

Bungwe la AU Liwonetsetsa kuti Zisankho Mmayiko amu Africa Zikuyenda Bwino

Bungwe la African Union (AU)  lati lili ndi udindo woonetsetsa kuti mabungwe oyendetsa zisankho m`mayiko a mu Africa ali ndi kuthekera koyendetsa zisankho  mwabata ndi mtendere.  M`modzi mwa akuluakulu...

View Article


Dziko la Guatemala Lichita Chisankho cha Pulezidenti

Anthu a mdziko la Guatemala achita chisankho chosankha mtsogoleri wina wa dzikolo. Chisakhochi chachitika mtsogoleri wa dzikolo a Perez Molina atatula pansi udindo wake komanso wamangidwa kamba koti...

View Article


Mneneri wa Chipani Chotsutsa cha UPD Mdziko la Burundi Waphedwa

Mneneri wa chipani china chotsutsa mdziko la Burundi waphedwa lolemba usiku atawomberedwa ndi anthu osadziwika mu mzinda wa Bujumbura.   Mneneriyu Patrice Gahungu anali wa chipani cha Union for Peace...

View Article

Papa Benedict wa 16 ndi Wokhudzidwa ndi Mavuto omwe Anthu Othawa Kwawo...

Mtsogoleri wampingo wakatolika wopuma Papa Benedict wa  16 ati ndi okhudzidwa ndi mavuto omwe anthu othawa kwawo chifukwa cha nkhondo komanso anthu omwe amachoka m`mayiko mwawo kamba kosowa ntchito,...

View Article

Chiwelengero cha Imfa za Ana Osakwana Zaka Zisanu Chatsika

Nthambi ya bungwe la United Nations lowona za Umoyo la World Health Organisation WHO lati chiwerengero cha imfa za  ana osakwana zaka zisanu  chatsika ndi mapereseti pafupifupi makumi asanu kuyambira...

View Article

Bungwe la CFM lakonza Msonkhano Wapachaka

Bungwe la mabanja a chikhristu mu  mpingo wakatolika la Christian Family Movement CFM lati lidzipereka kukonza mfundo zothandiza kupititsa moyo wa m’banja patsogolo. Mkulu wa bungweli m’chigawo cha...

View Article


Chikondwelero cha Radio Maria Choir Festival Chikhala Chopambana

Chikondwelero cha mayimbidwe cha  Radio Maria Malawi  ati chikhala chopambana kusiyana ndi momwe zinthu zakhala zikuyendera mmbuyomu. Wapampando wa komiti yoyendetsa chikondwelero cha mayimbidwe a...

View Article

Mabanja Abwino Angabweretse Chitukuko mu Mpingo ndi Mdziko

Mpingo wakatolika mdziko muno wati umazindikira kuti kukhala ndi mabanja  abwino kungathandize chitukuko cha mpingo komanso dziko.   Episkopi wa dayosizi ya Chikwawa Ambuye Peter Musikuwa ndi omwe...

View Article


Bambo Nsope Apempha Ophunzira a Sukulu ya Ukachenjede ya Chancellor Kukhala...

Ophunzira achikatolika ku Chancellor College mu mzinda wa Zomba awapempha kuti azikonda kulimbikitsa makhalidwe abwino ndi okonda kupemphera nthawi zonse.   Bambo Alfred Nsope ndi amene apereka...

View Article

Papa Francisco ndi Okhudzidwa ndi Mavuto omwe Anthu Othawa Kwao Akukumana Nawo

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse la pansi  Papa Francisco wati dziko lapansi likukumana ndi mavuto aakulu a anthu omwe akuthawa mmayiko awo kamba ka nkhondo,njala komanso kusowa kwa...

View Article


Apolisi Mdziko la Egypt Apha Anthu Khumi ndi Awiri

Apolisi mdziko la Egypt apha mwa ngozi anthu khumi ndi awiri kuphatikizapo nzika ya mdziko la Mexico yomwe imakayenda mdzikolo.   Anthuwo amayenda mugalimoto zinayi zomwe zinalowa kumalo ena...

View Article

Mnyamata Wazaka 17 Waba Njinga Yamoto M’boma la Ntchisi

Apolisi m’boma la Ntchisi amanga mnyamata wina wa zaka 17 zakubadwa yemwe akumuganizira kuti  waba njinga ya moto ya ndalama zosachepera 295 sauzande kwacha. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali...

View Article

Papa Francisco Wapempha Akhristu kuti Akhale Okonda Kuchita Ntchito za Chifundo

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu, kuti aziwonetsa chikhulupiliro chawo, pothandiza anthu ovutika komanso odwala matenda osiyanasiyana. Papa Francisco,...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>