Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

ANA ASUKULU ASAFIKE NTHAWI YOTSEKULIRA SUKULU ALI KU TSIMBA

$
0
0

Ofesi ya zamaphunziro m’boma la Balaka yati chaka chino iwonetsetsa kuti ana omwe alowe zinamwali, asakhale akadali kutsimba sukulu ikatsekulidwa mchigawo choyamba cha maphunziro a chaka chino mpaka chaka cha mawa. Mkulu owona za maphunziro m’bomalo a Paul Chiphanda ati ofesi yao, igwira ntchito limodzi ndi mafumu komanso makolo pofuna kuti m’chitidwewu uchepe chaka chino.Iye walankhula izi potsata kukula kwa chiwerengero  cha ana omwe abali asanatuluke ku tsimba nthawi yotsekulira sukulu itayamba chaka chatha.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>