Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Ndewu Pakati Pa Njoka ndi Chule

Ulaliki titled Ndewu Pakati Pa Njoka ndi Chule by Father James Chizuma

View Article


NZIKA ZILI NDI UDINDO PA ZISANKHO ZA 2014-MEC

Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC), lati nzika za m’dziko lino zikuyenera kuonetsa udindo wawo potenga mbali pazisankho zachaka cha mawa polembetsa m’nkaundula wa mavoti. Wapampando wa bugweli...

View Article


NYUMBA YA MALAMULO IVOMEREZA BOMA KUTENGA NGONGOLE YA 14.8 BILLION KWACHA

Nyumba ya malamulo mdziko lino yavomereza Boma kutenga ngongole ya ndalama zokwanira 14.8 billion kwacha zoti ligwiritsire ntchito yomangira msewu wa Mzuzu- Nkhatabay. Nduna ya za chuma Olemekezeka a...

View Article

A MANG'ANJA AKUMANA- CHILUKUNZAKO

Bungwe la anthu a mtundu wa a MANG’ANJA lati liri mkati mokonza dongosolo lofuna kukhaka ndi msonkhano waukulu wa anthu a mtundu-wu m'dziko muno. M’modzi mwa akuluakulu a bungweli m’dziko muno a PULENI...

View Article

Mundifatsire

Ulaliki titled Mundifatsire by Father E Nthalika

View Article


Bola Akadamwalira Dzana

Ulaliki titled Bola akadamwalira Dzana by Father E Nthalika

View Article

Ntchimo Limasaka Munthu

Ulaliki titled Ntchimo Limasaka Munthu by Father E Nthalika

View Article

ANA ASUKULU ASAFIKE NTHAWI YOTSEKULIRA SUKULU ALI KU TSIMBA

Ofesi ya zamaphunziro m’boma la Balaka yati chaka chino iwonetsetsa kuti ana omwe alowe zinamwali, asakhale akadali kutsimba sukulu ikatsekulidwa mchigawo choyamba cha maphunziro a chaka chino mpaka...

View Article


MEC IKHAZIKITSA NDONDOMEKO YA CHISANKHO CHA 2014

Bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission MEC latsimikizira  anthu kuti ligwira ntchito yake mwa ukadaulo komanso mwachilungamo  m’dziko muno. Wampando wa bungweli  Justice...

View Article


KWAYA ZIZAMITSE LUSO LOPEKA NYIMBO KUCHOKERA M'BUKU LOYERA

M’modzi mwa akatswiri poyimba nyimbo za uzimu m’dziko muno, PAUL BANDA wati mayimbidwe mu mpingo wakatolika, angapite patsogolo komanso kuyenda bwino, pokhapokha magulu oyimba  mu mpingowu atazamitsa...

View Article

AMAI A CHITEMWANO ACHEZERA ASEMINO KU KACHEBERE SEMINARY

Achinyamata omwe ali pamaphunziro aunsembe ku sukulu ya Kachebere m’boma la Mchinji, ayamikira gulu la amai la Chitemwano la mparishi ya St Denis ya mpingo wakatolika mudayosizi ya Mzuzu yampingowu,...

View Article

UMOYO PATSOGOLO

Sabata yathunthu yoganizira zaumoyo,yayamba lero mdziko muno pamene zipatala zalimbikitsa ntchito yopereka katemera wa Ana ndi zithandizo zina kwa ana osaposera zaka zisanu. Pothilirapo ndemanga...

View Article

APHUNGU AKUNYUMBA YA MALAMULO AYAMBA KUVOMERA KAPENA KUKANA BUDGET

Aphungu akunyumba yamalamulo masana ano ayamba kuvomera kupena kukana ndondomeko yazachuma yomwe nduna yazachuma idapereka kunyumbayo pa 24 mwezi watha.Pamkumanowu aphunguwa akhala akukana kapena...

View Article


CCJP IPHUNZITSA ZA KUSAMALIRA CHILENGEDWE

Bungwe la Catholic Commission for Justice and Peace mu arkdayosizi ya LILONGWE, lati ngati dziko lino silikhala tcheru ndikulimbikitsa mchitidwe osamalira zachilengedwe, lidzakumana ndizovuta zambiri...

View Article

NAPHAM IKONDWA NDI MAMEMBALA AKE KU MANGOCHI

Bungwe la National Association for People Living with HIV and AIDS (NAPHAM) m’boma la MANGOCHI lati ndi lokondwa kuti ena mwa mamembala ake ayamba kuchita bwino pa miyoyo yawo kamba kotsatira bwino...

View Article


KULUNGAMA SAPATSIRANA

New Ulaliki titled Kulungama Sapatsirana by George Makondi

View Article

PALIBE CHISANKHO CHACHIBWEREZA MU 2014 -MEC

Bungwe loyendetsa zisankho m'dziko muno, la Malawi Electoral Commission,lati silidaike tsiku lodzachitira chisankho chachibwereza m'ndondomeko yakagwiridwe ka ntchito zake zokonzekera chisankho cha...

View Article


MAFUMU ALI NDI UDINDO WOLIMBANA NDI MCHITIDWE WOZEMBETSA ANA

Bungwe losamalira ana la Chisomo Childrens Club lati lipitiriza kudzipereka polimbana ndi mchitidwe ozembetsa ana m'madera osiyanasiyana mdziko muno. Bungweli lanena izi m’boma la Dedza pamsonkhano...

View Article

MWAMUNA WINA ALAMULIDWA KUKHALA KUNDENDE ZAKA 8 ATABA MATUMBA 202 A FETEREZA

Bwalo la milandu la magistrate m'boma la Ntchisi lalamula mwamuna wina wa zaka 27, kuti akakhale kundende zaka zisanu ndi zitatu (8), atapezeka olakwa pa mlandu woba fetereza ndi mbewu za ndalama...

View Article

ATSOGOLERI ALEPHERA PA CHUMA - JUBILEE 50 MOVEMENT

Gulu lina la achinyamata lomwe langokhazikitsidwa kumene la JUBILLEE 50 MOVEMENT, lati atsogoleri omwe akhala akulamulira dziko lino alephera kukwaniritsa kukweza ntchito za chuma m'dziko muno....

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>