Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

MEC IKHAZIKITSA NDONDOMEKO YA CHISANKHO CHA 2014

$
0
0

Bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission MEC latsimikizira  anthu kuti ligwira ntchito yake mwa ukadaulo komanso mwachilungamo  m’dziko muno.

Wampando wa bungweli  Justice Maxson Mbendera ndi yemwe walankhula izi pa mwambo wokhazikitsa ndondomeko ya momwe bungweli ligwilire ntchito zake pokonzekera chisankho cha chaka cha mawa chomwe chidzakhale cha Aphungu, Pulezidenti komanso Makhansala. Justice Mbendera  wati  bungwe la MEC sililamulidwa ndi munthu aliyense kuphatikizapo boma kotero kuti ligwira ntchito yake mokomera anthu onse.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>