Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

ECM Yasankha Bambo Likutcha Kukhala Mlangizi wa Apolisi

$
0
0

Bungwe la ma episkopi mdziko muno la Episcopal Conference Of Malawi [ECM] lasakha Bambo Steven Likhucha kukhala  mlangizi wa apolisi  mumpingowu m’dziko muno.

Bungweli  lanena izi kudzera muchikalata chomwe latulutsa ndipo chasainidwa ndi mlembi wa bungweli Bambo Henry Saindi.

Bambo Likhutchaalowa m`malo mwa Bambo David Bello, omwe anapuma zaka zawo zokhalira paudindowu zitatha.

Kalatayi yatinso Bambo Likhutcha omwe ndi wamsembe otumikira  ku dayosizi ya Zomba ayamba kugwira ntchito paudindowu pa 30 June chaka chino.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko