Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Akhristu 49 akuno ku Malawi ankhala nawo pa Mwambo wa Misa Wokumbukila...

Akhristu 49 a mpingo wakatolika akuno ku Malawi, lachitatu anakhala nawo pamwambo wamapemphero okumbukira a maritiri 22 ku Namugongo Shrine mdziko la Uganda. Mmodzi mwa amaritiriwa Charles Lwanga Oyera...

View Article


Chiwelengelo cha Akhristu Achikatolika Chikukula

Lipoti lomwe nthambi yowona zakafukufuku pa sukulu ina ya ukachenjede mdziko la America yatulutsa lati chiwerengero cha akhristu a mpingo wakatolika padziko lonse chikukwera kwambiri maka mmaiko a mu...

View Article


Cadecom Inkhazikitsa Tchito Yonthandiza Anthu Mboma la Chikhwawa.

Dayosizi ya mpingo wakatolika ya Chikhwawa yati iwonetsetsa kuti ntchito za Bungwe lowona zachitukuko mumpingowu la CADECOM zikupindulira anthu onse mu Dayosiziyo. Episikopi wa Dayosiziyi  wolemekezeka...

View Article

Apolisi M’dziko la New Guinea Akuwaganizira Kuti Apha Ophunzira Anayi Omwe...

Apolisi m’dziko la New Guinea akuwaganizira kuti apha ophunzira anayi   a pa sukulu ina ya ukachenjede omwe amachita chionetsero chosonyeza kusakondwa ndi zochita za nduna yaikulu ya dzikolo. Malingana...

View Article

Anthu Makumi Atatu Afa Zigawenga za Islamic State Zitaphulitsa Bomba La Timke...

Anthu makumi atatu afa, ndipo ena 80 avulala  gulu la zigawenga la Islamic State litaphulitsa  mabomba awiri atinkenawo  munzinda wa Baghdad  m`dziko la Iraq Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, bomba...

View Article


ECM Yasankha Bambo Likutcha Kukhala Mlangizi wa Apolisi

Bungwe la ma episkopi mdziko muno la Episcopal Conference Of Malawi [ECM] lasakha Bambo Steven Likhucha kukhala  mlangizi wa apolisi  mumpingowu m’dziko muno. Bungweli  lanena izi kudzera muchikalata...

View Article

Kanyongolo Wapempha Boma Libwezeretse Maubale Ndi Maiko Ena

Katswiri wa malamulo yemwenso ndi mphunzitsi wa malamulo pa sukulu ya ukachenjende ya Chancellor, Professor Edge Kanyongolo wapempha boma  kuti libwezeretse ubale womwe unasokonekera pakati pa boma la...

View Article

Polisi ya Kanengo Iyenda Ulendo Wandawala Pofuna Kuzindikiritsa Anthu za...

Ngati njira imodzi yotenga  nawo gawo pa ntchito yothana ndi m`chitidwe wopha anthu a mtundu wa chi alubino, apolisi a Kanengomu m’zinda wa Lilongwe akonza  ulendo wa ndawala womwe cholinga chake...

View Article


Alshabaab Yapha Asilikali Makumi Anayi a AU ku Somalia

Gulu la zigawenga la  Al-Shabaab  lati lapha   asilikali okwana  makumi anayi  pachiwembu  chomwe linachita  kumalo a asilikali  a African Union   m`chigawo chapakati pa dziko la Somalia. Bungwe la...

View Article


Mgwirizano wa Apolisi ndi Amalonda Ungapititse Patsogolo Chitetezo cha Dziko...

Chitetezo cha dziko lino ati chingalimbikitsidwe ngati pali ubale wabwino pakati pa apolisi ndi anthu amalonda. Wachiwiri kwa mkulu wa apolisi ya Bvumbwe , SupretendantMoses Katanda walankhula izi ndi...

View Article

Abungwe la Amayi Akatolika Akonzekere Bwino Msonkhano wa Padziko Lonse

Amayi ampingo wakatolika mdziko muno awapempha akuti adzipeleke pa ntchito yokonzekera msonkhano wawo wapaziko lonse umene udzachike mwezi wa September m’dziko muno. Msonkhanowu ndi wa amayi pa dziko...

View Article

MOAM Ipempha Boma Liwunikenso Misonkho

Bungwe la eni minibus m`dziko muno la Minbus Owners Association of Malawi(MOAM) lapempha boma kuti liwunikenso  misonkho pofuna kuti ikhale yokomera anthu  ochita malonda ang’onoang’ono omwe ambiri...

View Article

Mkulu wa Bungwe la Community of Saint Egidio Mdziko Muno Wamwalira

Bungwe la Community of Saint Egidio lati lili mkati mokonza dongosolo la mwambo woyika m'manda yemwe anali mkulu wa bungweli m'dziko muno a Ellard Alumando. Malemu-yi Ellard Alumando anamwalira masiku...

View Article


Achinyamata Azigwiritsa Bwino Ntchito Luso la Makono Pofalitsa Uthenga wa...

Achinyamata a bungwe la Young Christian Workers (YCW) mumpingo wa katolika  awalangiza kuti azigwiritsa  bwino ntchito maluso atsopano omwe akubwera mdziko muno  monga ma computer komanso internet...

View Article

Ma Episkopi Apempha Mzika Kuti Zipempherere Dziko la Nigeria Pofuna Kuthetsa...

Bungwe la ma episkopi mdziko la Nigeria la Catholic Bishops’ Conference of Nigeria lapempha  mzika za dzikolo kuti zipitilize kupemphelera dzikolo pofuna kuthana ndi mchitidwe wa katangale komanso...

View Article


Boma Lati Lipereka Chilango Chokhwima kwa Opezeka ndi Mlandu Wopha ma Alubino

M’tsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati boma lake lionetsetsa kuti aliyense wopezeka ndi mulandu wakupha kapena kuchitira nkhanza anthu a mtundu wa chi Alubino m’dziko muno...

View Article

Eye Of The Child Ikhazikitsa Bukhu Lozindikiritsa Mavuto Omwe Ana Amakumana Nawo

Bungwe la Eye ofthe Child m’dziko muno lalemba bukhu lomwe lili ndi mfundo zothandiza kuzindikira mavuto omwe ana amakumana nawo monga kugwililidwa mosavuta.   Polankhula ndi Radio Maria Malawi, mkulu...

View Article


Dziko la Malawi Lichita Mwambo wa Tsiku Loganizira Mchitidwe Wogwiritsa Ana...

Dziko la Malawi lachisanu lichita mwambo wa tsiku loganizira m’chitidwe woyipa wogwilitsa ntchito ana (World Day Against Child Labour). Dziko la Malawi lidzachita mwambowu pogwilizana ndi mayiko pa...

View Article

Mfumu Kachule Ikulimbikitsa Maphunziro Kwa Ana Mdera Lake

Mfumu Kachule ya m’dera la mfumu yayikulu Kachere m’boma laDedza yati ipitiliza kudzipeleka pa chisamaliro ndi chitetezo cha ana a m’dera lake ndi cholinga choti azikhala ndi kukula ndi makhalidwe...

View Article

Bungwe la Episcopal Conference of Malawi Liri ndi Mlembi Watsopano.

Mlembi watsopano wabungwe la maepiskopi mdziko muno la Episcopal conference of Malawi Bambo Henry Saindi ati apitiliza kudzipereka potumikira Mulungu pogwiritsa ntchito mphatso zomwe ali nazo pofunanso...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>