Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

CCJP IPHUNZITSA ZA KUSAMALIRA CHILENGEDWE

$
0
0

Bungwe la Catholic Commission for Justice and Peace mu arkdayosizi ya LILONGWE, lati ngati dziko lino silikhala tcheru ndikulimbikitsa mchitidwe osamalira zachilengedwe, lidzakumana ndizovuta zambiri mtsogolo, maka zokhudza kusintha kwa nyengo.

Bungweli lati nchifukwa chake,layamba ntchito yophunzitsa ana msukulu zapulayimale m`boma la Salima pa momwe angasamalirire zachilengedwe ndikuonetsetsa kuti mavuto azakusintha kwa nyengo,asadzafike povuta mdziko muno.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>