Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Ma Episkopi Adzudzula Apolisi Mdziko la Phillipines

$
0
0

Bungwe la maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la Philippines la Catholic Bishops Conference of the Philippines   ladzudzula apolisi mdzikolo kamba ka mchitidwe wakupha anthu a mdzikolo omwe akuwaganizira milandu yosiyanasiyana.

Malinga ndi kalata yomwe bungweli latulutsa maepiskopiwa ndi okhudzidwa ndi kukwera kwa chiwerengero cha anthu omwe akuphedwa kaamba kopalamula milandu yosiyanasiyana mdzikolo ati kaamba koti akumakana kumangidwa.

Kalatayi yati ngakhale zili zololedwa kupha munthu pofuna kudziteteza, apolisiwa sakuyenera kupha anthu oganiziridwa  kaamba kofuna kulandira ndalama.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>