Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Chaka cha Achinyamata pa Dziko Lonse 2019 Chidzachitikira Mdziko la Panama

$
0
0

Mpingo wakatolika m’dziko la Panama wati ndi wokondwa ndi uthenga umene walandira woti chaka cha achinyamata mu mpingowu pa dziko lonse chidzachitikire  mdzikomo.

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco ndi amene walengeza zoti chaka cha achinyamata chomwe mpingowu udzachitenso mchaka cha 2019 chidzachitikire mu dayosizi ya mpingowu ya Panama.

Papa wanena izi pakutha pa mwambo wotsekera chaka cha achinyamata chomwe chimachitikira ku Krakow m’dziko la Poland. Pothilira ndemanga Arch-Bishop Jose Domingo Ulloa Mandieta wa arch-dayosizi ya Panamam’dzikomo wati mpingo wakatolika ndi wokondwa ndi uthenga-wu ndipo ukhale ukukonzekera bwino chakachi.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>