Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Boma Lichite Kafukufuku Okhudzana ndi Kupsa kwa Misika

$
0
0

Bungwe lomenyera ufulu wa anthu mdziko muno la Human Rights Defender lapempha boma kuti lichite kafukufuku okwanira okhuzana ndi kupsa kwa misika m’dziko muno.

Mkulu wa bungweli a Billy Mayaya ndi omwe anena izi polankhula ndi Radio Maria Malawipotsatira kupsa kwa msika wa mu mzinda wa Lilongwe.

Iwo ati akudabwa kuti mpaka pano boma silikupereka yankho pa zakupsa kwa misika m’dziko muno zomwe ati zikupereka chiopsezo kwa anthu omwe amadalira malonda.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>