Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

“Tidzidalire pa chitukuko” Bwanamkubwa.

$
0
0

Anthu m’boma la Mwanza awapempha kuti adzizidalira pantchito ndi cholinga chotukula miyoyo yawo komanso kupititsa patsogolo chitukuko cha dziko lino.

Bwanankubwa wa Bomalo a Gift Rapozo ndiomwe analakhula izi pa mwambo wogawa mbuzi kwa alimi omwe bungwe la Malawi Interfaith  Aids Association (MIA) linapereka m’bomalo.

“Anthu olimbikira okha ndi amene angathe kupindula patchito zachitukuko zomwe zingathandize kupititsa patsogolo chuma cha dziko lino”. atero a Rapozo.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>