Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

OPHUNZIRA MSUKULU ZOSIYANASIYANA APHUNZITSIDWE ZA CHILENGEDWE

Unduna woona zachilengedwe ndi kusintha kwa nyengo wati ugwira ntchito ndi unduna wa zamaphunziro ndi cholinga choti ophunzira m’sukulu zosiyanasiyana aziphuzitsidwa mokwanira momwe angamasamalire...

View Article


Akhristu ku America akukonda kwambiri Papa Francis

Kafukufuku wina yemwe akuluakulu ena achita m’dziko la America akuti akuwonetsa kuti akhristu  ambiri a mpingo wa Katolika akukonda mtsogoleri wa mpingowu pa dziko lonse Papa Francis. Ngakhale kuti...

View Article


Boma lipitiriza kulanda maukonde osavomerezeka kuphera nsomba ku Nyanja ya...

Boma lati lipitiriza kulimbikitsa kampeni yoteteza nsomba polanda maukonde osavomerezeka kuchokera kwa asodzi pofuna kuthana ndi mchitidwe wochita usodzi mosatsatira malamulo omwe ukuchititsa kuti...

View Article

“Tidzidalire pa chitukuko” Bwanamkubwa.

Anthu m’boma la Mwanza awapempha kuti adzizidalira pantchito ndi cholinga chotukula miyoyo yawo komanso kupititsa patsogolo chitukuko cha dziko lino. Bwanankubwa wa Bomalo a Gift Rapozo ndiomwe...

View Article

Bungwe la MEC latsutsa zoti likumayika zipangizo zosagwira bwino ntchito ku...

Bungwe lowona zachisankho la Malawi Electoral Commission MEC latsutsa malipoti oti likumayika zipangizo zosagwira bwino ntchito pa kalembera wa zisankho ku malo komwe anthu ena akuganiza kuti ndi komwe...

View Article


Mipingo ndi zipembedzo zakhazikitsa ndondomeko yothandiza kuti zisankho...

Magulu azipembedzo zosiyanasiyana  mdziko muno atsekulira ntchito yomwe akuyitcha Interfaith Elections Initiative ngati njira imodzi yothandizira kuti zisankho za chaka cha mawa zidzayende bwino....

View Article

On 30th September we will know the canonisation date of the Popes- JOHN XXIII...

The Consistory will meet on Monday 30th September when Pope Francis will announce the canonization date for the two Pontiffs. Blessed John XXIII (aka Angelo Giuseppe Roncalli) was elected Pope on 28th...

View Article

THE POPE WILL PAY HOMAGE TO ST. FRANCIS

On 4th October this year, the day on which we remember the patron saint of Italy, Saint Francis, Pope Bergoglio will visit Assisi to pay homage to the place in which the son of the rich merchant Pietro...

View Article


Radio Maria with the Pope for Peace

One of the cornerstones of the identity of Radio Maria is faithfulness to the Magisterium which becomes tangible not only in the editorial policy, but also in the special attention with which the key...

View Article


CHIPANI CHA PPM CHIPIKISANA NAWO PA UPRESIDENT

Chipani cha People’s Progressive Movement PPM chati chidzapikisana nawo pa mpando wa Upresident pa  zisankho za chaka cha mawa kaamba koti chili ndi mfundo zake za tsopano zomwe zidzathandize pa...

View Article

OPHUNZIRA A VUTO LAKUSAWONA APEMPHA ZIPANGIZO ZA BRAIL KUTI ADZAVOTE BWINO.

Ophunzira omwe ali ndi vuto lakusawona  pa sukulu ina m'boma la Mulanje  apempha bungwe la Malawi Electoral Commission MEC kuti liwapititsire  zipangizo za Brail kuti iwo adzathenso ku vota bwino  pa...

View Article

“Makhansala achepetsa ntchito za mafumu” T/A Nkangula

Sub T/A Nkangula ya m'boma la Zomba yati kusankhidwa kwa makhansala pa zisankho za chaka cha mawa kuthandiza kuchepetsa ntchito yomwe mafumu akhala akugwira zomwe zithandize pa chitukuko cha dziko...

View Article

BUNGWE LA MEC LIDZITSEKULANSO MALO AKALEMBERA ENA PAKAKHALA MAVUTO ENA

Bungwe lowona za chisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lati litsekulanso malo ena olembetsera kalembera wa zisankho ku malo omwe anthu sanathe kulembetsa kwa masiku 14 kamba ka mavuto ena....

View Article


ZIWONETSERO ZOKWIYA NDI BOMA MUMZINDA WA BLANTYRE

Pamene kwangotsala miyezi yowerengeka kuti dziko lino lichititse chisankho cha pulezidenti mabungwe omwe siaboma pansi pa mgwirizano wawo olimbikitsa nkhani za demokalase ndi ulamuliro wabwino mdziko...

View Article

MAPHUNZIRO A MAWU A MULUNGU A LERO

Kukhala maphunziro kwa onse amene amawerenga Mawu a Mulungu a lero pa Radio Maria ku Limbe Cathedral ku Blanyre loweruka pa 1 March 2014 nthawi ya 8 koloko mmawa. Pobwera atenge zinthu izi, Baibulo,...

View Article


OPHUNZIRA AM'SUKULU ZASEKONDALE APINDULA NDI DSTV

Kampani ya Multi Choice Malawi yati ophunzira a m’sukulu zasekondale zomwe sizaboma tsopano ali ndi mwayi opindula nawo kudzera ku mapologalamu awulele othandiza pamaphunziro omwe amawonetsedwa pa...

View Article

ANTHU AKU CHIKHWAWA AKUKAKAMIZA MFUMU YAWO KUTI ITULE PANSI UDINDO

Anthu a mdera la mfumu Ngowe m’boma la Chikhwawa awopseza kuti achita ziwawa ngati  boma siliwathandiza pa nkangano wawo ndi mfumu Ngowe yomwe ati yakhala ikugulitsa minda yawo kwa anthu andale komanso...

View Article


BAMBO APEZEKA NDI MAFUPA A MUNTHU KU MANGOCHI

Bwalo la magistrate ku Namwera mboma la Mangochi lalamula mzika ya zaka 37 ya mdziko la Mozambique, Jairosi Duwa kukakhala kundende chifukwa chopezeka ikugulitsa mafupa a munthu kwa munthu wina...

View Article

92 BILIYONI KWACHA INABEDWA MCHAKA CHA 2010-JB

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Joyce Banda wati kafukufuku wapeza kuti ndalama pafupifupi 92 biliyoni kwacha za boma zinasowa m'chaka cha 2010 mu ulamuliro wachipani cha Democratic Progressive (DPP)....

View Article

NDUNA YA ZA UMOYO YATI KUNYALANYAZA KWA OGWIRA NTCHITO KUNAWONGETSA MATUPI A...

Nduna ya za umoyo mayi Catherine Gotani Hara, ati kunyalanyaza kwa akulu akulu apachipatala cha Kamuzu Central mu mzinda wa Lilongwe ndi komwe kunachititsa kuti matupi ochuluka a anthu awonongeke ku...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>