Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Apempha Wailesi Zifalitse Nthenga Wothetsa Kufala Kwa Kolera

$
0
0

Nyumba zowulutsa mawu za m’madera a kumidzi (Community Radio) azipempha kuti zizipereke pa ntchito yofalitsa mauthenga a njira zopewera matenda a kolera omwe amafala kwambiri mu nyengo ya mvula.

Mmodzi mwa akuluakulu mu unduna wa zaumoyo mdziko muno a Elton Chidothi Banda anena izi m’boma la Kasungu potsekera maphunziro a tsiku limodzi othandiza atolankhani  za udindo wawo pa ntchito zolimbana ndi kufala kwa matendawa mdziko muno.

A Banda ati ngakhale kuti dziko lino likuchita bwino polimbana ndi matenda a kolera, ma wailesi akuyeneranso kupitiriza kumwaza mauthenga kuti mbiri ya kupezeka kwa matendawa ikhale ya makedzana.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko