Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Anthu 10 Afa ndi Bomba Mdziko la Somalia

$
0
0

Anthu khumi (10) afa ndipo ena avulala   anthu ena ataphulitsa mabomba awiri pa chipata cholowera kubwalo la ndege mu mzinda wa Mogadishum`dziko la Somalia.

Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, anthu omwe afawo ambiri ndi achitetezo chapamalopo. Atolankhani a m`dzikolo ati bomba loyamba linali la tinkenawo ndipo lina ati laphulika pafupi ndi khoma lalikulu ku bwalo la ndegero.

Pakadali pano gulu la zigawenga za Al-Shabaab lati ndilo lachita chiwembuchi.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>