Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Parish Ya Bango Ku Mulanje Ichita Chaka Cha Zaka 50 Za Parishi-yi.

$
0
0

Mwambo wokondwelera kuti parish ya Bango ku Mulanje mu arch-dayosizi ya Blantyre kuti yakwanitsa zaka 50 chiyikhadzikitsileni udzachitika pa 3 mwezi wa June chaka chino.

Wapampando wa komiti yomwe ikuyendetsa mwambowu a Martha Khembo ndi omwe anena izi pofotokozera mtolankhani wathu amene amafuna kudziwa zambiri zokhudza chakachi.

Iwo ati akhristu akuyenera kudzafika mwa unyinji wawo kuti mwambowu udzakhele wopambana.


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>