Quantcast
Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Anthu 200 Aphedwa Mdziko La Syria

Anthu wamba oposera 200 ndi omwe afa mdziko la Syria kaamba ka mabomba ochokera mu ndege za asilikali a mdziko la America kuyambira pa 23 April kufikira pano.

Malinga ndi malipoti a News 24 bungwe lowona za maufulu a anthu mdzikolo litachita kafukufuku lapeza kuti mwa anthuwa makumi asanu ndi atatu 80 ndi ana komanso amayi.

Asilikali a mdziko la America anayamba kuponya mabomba mdziko la Syria mmwezi wa September chaka cha 2014 pofuna kuthana ndi gulu la zigawenga la chisilamu la Jihadists. 


Viewing all articles
Browse latest Browse all 1875

Trending Articles


Mdima unadetsa dziko



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>